BOKOSI 11A
Alonda Ena Achitsanzo Chabwino
Alondawo ankatsutsidwa koma anakhalabe okhulupirika ndipo ankalengeza uthenga wochenjeza komanso wabwino.
ISIRAELI WAKALE
-
Yesaya 778–cha m’ma 732 B.C.E.
-
Yeremiya 647-580 B.C.E.
-
Ezekieli 613–cha m’ma 591 B.C.E.
NTHAWI YA ATUMWI
-
Yohane M’batizi 29-32 C.E.
-
Yesu 29-33 C.E.
-
Paulo cha m’ma 34–cha m’ma 65 C.E.
MASIKU ANO
-
C. T. Russell ndi anzake cha m’ma 1879-1919
-
Kapolo Wokhulupirika 1919–Mpaka lero