BOKOSI 22A
Kukumana ndi Mayesero Omaliza
-
Anthu Adzakhalanso Angwiro—1 AKOR. 15:26
-
Yesu Adzapereka Ufumu kwa Yehova—1 AKOR. 15:24
-
Satana Adzamasulidwa Kuchokera Kuphompho; Anthu Opanduka Adzakhala Kumbali ya Satana pa Kuukira Komaliza—CHIV. 20:3, 7, 8
-
-
Anthu Adzakhala ndi Moyo Wosatha, Mwamtendere Komanso Mogwirizana—AROMA 8:19-21