BOKOSI 10A
Kulambira Koyera—Kunabwezeretsedwa Pang’onopang’ono
-
“Gobedegobede”
William Tyndale ndi anzake anamasulira Baibulo m’Chingelezi komanso m’zilankhulo zina
-
“Mitsempha ndi mnofu”
Charles T. Russell ndi anzake anabwezeretsa choonadi cha m’Baibulo
-
“Iwo anakhala ndi moyo ndipo anaimirira”
Anthu a Yehova ‘atakhala ndi moyo’ mu 1919, anayamba kugwira ntchito yolalikira mwakhama