BOKOSI 12A
Kuphatikiza Ndodo Ziwiri
Yehova anauza Ezekieli kuti alembe pa ndodo imodzi kuti “ndodo ya Yuda” komanso pa ndodo ina alembe kuti “ndodo ya Yosefe yoimira Efuraimu.”
“ndodo ya Yuda”
KALE
Ufumu wa Yuda wa mafuko awiri
MASIKU ANO
Odzozedwa
“ndodo ya Yosefe yoimira Efuraimu”
KALE
Ufumu wa Isiraeli wa mafuko 10
MASIKU ANO
Nkhosa zina
“zikhale ndodo imodzi mʼdzanja lako”
KALE
537 B.C.E. Anthu amene ankalambira Mulungu woona anabwera kuchokera m’mitundu yosiyanasiyana, anamanganso Yerusalemu ndipo anayamba kulambira Yehova monga mtundu umodzi.
MASIKU ANO
Kuyambira mu 1919, anthu a Mulungu pang’ono ndi pang’ono akugwirizananso kuti azitumikira Mulungu ngati “gulu limodzi.”