Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

BOKOSI 6A

“Umete Tsitsi Lako Ndi Ndevu Zako”

“Umete Tsitsi Lako Ndi Ndevu Zako”

Zimene Ezekieli anachita zinasonyeza zinthu zomwe zinali zitatsala pang’ono kuchitika mu Yerusalemu

  • “Umete”

    Ayuda adzaukiridwa ndipo adzawonongedwa

  • ‘Uyeze Tsitsi, Ukatero Uligawe’

    Chiweruzocho adzachita kuchikonzekera ndipo adzachipereka mwadongosolo

  • ‘Uliwotche’

    Anthu ena adzafera mumzindawo

  • “Nʼkumalimenya”

    Anthu ena adzaphedwa kunja kwa mzindawo

  • ‘Uliuluze’

    Anthu ena adzathawa koma sadzapeza mtendere

  • “Nʼkulikulunga”

    Anthu ena amene anali ku ukapolo adzabwerera ku Yerusalemu ndipo adzateteza kulambira koyera