Ziwerengero Zonse za 2018
Nthambi za Mboni za Yehova: 87
Mayiko Amene Anatumiza Lipoti: 240
Mipingo Yonse: 119,954
Opezeka pa Chikumbutso Padziko Lonse: 20,329,317
Amene Anadya Zizindikiro Padziko Lonse: 19,521
Ofalitsa Onse Amene Anagwira Ntchito Yolalikira *: 8,579,909
Avereji ya Ofalitsa Amene Ankalalikira Mwezi Uliwonse: 8,360,594
Kuwonjezeka kwa Ofalitsa Kuchokera mu 2017: 1.4
Obatizidwa Onse *: 281,744
Avereji ya Apainiya * Okhazikika Mwezi Uliwonse: 1,267,808
Avereji ya Apainiya Othandiza Mwezi Uliwonse: 446,642
Maola Onse Amene Tinalalikira: 2,074,655,497
Avereji ya Maphunziro a Baibulo * Mwezi Uliwonse: 10,079,709
M’chaka cha utumiki cha 2018, * a Mboni za Yehova anagwiritsa ntchito ndalama zoposa madola 214 miliyoni a ku America posamalira apainiya apadera, amishonale ndi oyang’anira dera pa utumiki wawo. Padziko lonse pali abale ndi alongo okwana 20,331 amene akutumikira m’maofesi a nthambi. Onsewa ali m’Gulu Lapadziko Lonse la Atumiki Apadera a Nthawi Zonse a Mboni za Yehova.
^ ndime 7 Wofalitsa ndi munthu amene amalalikira mwakhama uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu. (Mateyu 24:14) Kuti mudziwe mmene timapezera chiwerengerochi, onani nkhani ya pa jw.org yakuti “Kodi a Mboni za Yehova Alipo Angati Padziko Lonse?”
^ ndime 10 Kuti mudziwe zimene mungachite kuti mubatizidwe n’kukhala wa Mboni za Yehova, onani nkhani ya pa jw.org yakuti “Kodi Ndingatani Kuti Ndikhale wa Mboni za Yehova?”
^ ndime 11 Mpainiya ndi wa Mboni wachitsanzo chabwino amene amadzipereka kuti azilalikira uthenga wabwino kwa maola enaake mwezi uliwonse.
^ ndime 14 Kuti mudziwe zambiri, onani nkhani ya pa jw.org yakuti “Kodi Phunziro la Baibulo N’chiyani?”
^ ndime 15 Chaka chautumiki cha 2018 chinayamba pa September 1, 2017, ndipo chinatha pa August 31, 2018.