Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Ziwerengero Zonse za 2019

Ziwerengero Zonse za 2019
  • Nthambi za Mboni za Yehova: 87

  • Mayiko Amene Anatumiza Lipoti: 240

  • Mipingo Yonse: 119,712

  • Opezeka pa Chikumbutso Padziko Lonse: 20,919,041

  • Amene Anadya Zizindikiro Padziko Lonse: 20,526

  • Ofalitsa Onse Amene Anagwira Ntchito Yolalikira *: 8,683,117

  • Avereji ya Ofalitsa Amene Ankalalikira Mwezi Uliwonse: 8,471,008

  • Kuwonjezeka kwa Ofalitsa Kuchokera mu 2018: 1.3

  • Obatizidwa Onse *: 303,866

  • Avereji ya Apainiya * Okhazikika Mwezi Uliwonse: 1,277,738

  • Avereji ya Apainiya Othandiza Mwezi Uliwonse: 464,980

  • Maola Onse Amene Tinalalikira: 2,088,560,437

  • Avereji ya Maphunziro a Baibulo * Mwezi Uliwonse: 9,618,182

M’chaka cha utumiki cha 2019, * a Mboni za Yehova anagwiritsa ntchito ndalama zoposa madola $224 miliyoni posamalira apainiya apadera, amishonale ndi oyang’anira dera pa utumiki wawo. Padziko lonse pali abale ndi alongo okwana 20,858 amene akutumikira m’maofesi a nthambi. Onsewa ali m’Gulu Lapadziko Lonse la Atumiki Apadera a Nthawi Zonse a Mboni za Yehova.

^ ndime 7 Wofalitsa ndi munthu amene amalalikira mwakhama uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu. (Mateyu 24:14) Kuti mudziwe mmene timapezera chiwerengerochi, onani nkhani ya pa jw.org yakuti “Kodi a Mboni za Yehova Alipo Angati Padziko Lonse?”

^ ndime 10 Kuti mudziwe zimene mungachite kuti mubatizidwe n’kukhala wa Mboni za Yehova, onani nkhani ya pa jw.org yakuti “Kodi Ndingatani Kuti Ndikhale wa Mboni za Yehova?”

^ ndime 11 Mpainiya ndi wa Mboni wachitsanzo chabwino amene amadzipereka kuti azilalikira uthenga wabwino kwa maola enaake mwezi uliwonse.

^ ndime 14 Kuti mudziwe zambiri, onani nkhani ya pa jw.org yakuti “Kodi Phunziro la Baibulo N’chiyani?”

^ ndime 15 Chaka chautumiki cha 2019 chinayamba pa 1 September 2018, ndipo chinatha pa 31 August 2019.