Kukhulupirika
Sl 18:25; Lu 1:74, 75; Aef 4:24; Chv 15:4
Onaninso Sl 116:15; 145:17
Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:
Ru 1:16, 17; 3:10—Rute anatsimikiza mtima kuti akhalabe wokhulupirika kwa Naomi komanso kwa Yehova
2Mf 2:1, 2, 4, 6—Elisa anatsimikiza mtima kuti akhala wokhulupirika kwa mneneri Eliya