Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
Kodi ndi ndani amene angatipatse mphamvu? (Yos. 1:9; Sal. 68:35)
Kodi tingatani kuti tipitirize kulimbitsa chikhulupiriro chathu? (Aheb. 11:6)
Kodi tikudziwa bwanji kuti tikhoza kugwira bwino ntchito imene Yehova watipatsa? (Hag. 2:4-9)
Kodi Yehova amatithandiza bwanji tikakumana ndi mavuto aakulu? (Sal. 18:6, 30; Akol. 4:10, 11)
N’chiyani chingathandize achinyamata komanso anthu amene ali pa banja kuti azikhala kumbali ya Yehova? (Mat. 22:37, 39)
Kodi tingatani kuti ‘tikhale olimba m’chikhulupiriro komanso amphamvu’? (1 Akor. 16:13; Aroma 15:5; Aheb. 5:11–6:1; 12:16, 17)