Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
Kodi tingasonyeze bwanji kuti timakonda Mulungu? (Deut. 13:3, 4; 1 Yoh. 5:3)
N’chifukwa chiyani tiyenera kukonda abale athu? (1 Yoh. 4:11, 20, 21)
Kodi tingasonyeze bwanji kuti timakonda anthu anzathu? (Lev. 19:18; Aef. 5:29)
Kodi tingatsanzire bwanji chikondi cha Yehova? (1 Pet. 4:8; Akol. 3:13)
Kodi tingatani kuti tizitamanda Yehova? (Sal. 104:33; 146:2, 5)
Kodi kukonda Yehova ndi mtima wathu wonse kumatanthauza chiyani? (Eks. 34:14; Amosi 5:15; Aroma 12:11)