Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Yambani Kuwerenga Baibulo

Yambani Kuwerenga Baibulo

Mukhoza kumasangalala powerenga Baibulo. Mfundo zotsatirazi zikuthandizani kudziwa mmene mungayambire. Sankhani nkhani imene ikukusangalatsani kenako werengani malemba omwe asonyezedwawo.

Anthu Otchuka Komanso Nkhani Zawo

Nzeru Zothandiza pa Moyo Wathu

Nkhani Zomwe Zingakuthandizeni . . .

Zimene Baibulo Limanena pa Nkhani ya . . .

ZIMENE ZINGAKUTHANDIZENI: Kuti muone nkhani yonse, muziwerenga chaputala kapena machaputala onse osati kungowerenga mavesi omwe asonyezedwa okhawo. Chongani chaputala chilichonse chomwe mwamaliza kuwerenga pogwiritsa ntchito tchati chakuti, “Chongani Machaputala Omwe Mwawerenga” chimene chili kumapeto kwa bukuli. Khalani ndi cholinga chowerenga Baibulo tsiku lililonse.