Lamlungu
“Limba mtima ndipo uchite zinthu mwamphamvu. Yembekezera Yehova”—SALIMO 27:14
M’MAWA
-
9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo
-
9:30 Nyimbo Na. 73 ndi Pemphero
-
9:40 NKHANI YOSIYIRANA: Kutsogoloku Tidzafunika Kulimba Mtima
-
Akadzalengeza Kuti “Bata ndi Mtendere!” (1 Atesalonika 5:2, 3)
-
Babulo Wamkulu Akamadzawonongedwa (Chivumbulutso 17:16, 17)
-
Polengeza Uthenga Wokhala Ngati Matalala (Chivumbulutso 16:21)
-
Gogi wa Kudziko la Magogi Akamadzaukira Anthu a Mulungu (Ezekieli 38:10-12, 14-16)
-
Pa Aramagedo (Chivumbulutso 16:14, 16)
-
Pokonzanso Dziko Lapansili (Yesaya 65:21)
-
Pa Mayesero Omaliza (Chivumbulutso 20:3, 7, 8)
-
-
11:10 Nyimbo Na. 8 ndi Zilengezo
-
11:20 NKHANI YA ONSE: Kodi Chiyembekezo Chakuti Akufa Adzauka Chimatithandiza Bwanji Kukhala Olimba Mtima? (Maliko 5:35-42; Luka 12:4, 5; Yohane 5:28, 29; 11:11-14)
-
11:50 Phunziro Lachidule la Nsanja ya Olonda
-
12:20 Nyimbo Na. 151 ndi Kupuma
MASANA
-
1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo
-
1:45 Nyimbo Na. 5
-
1:50 VIDIYO: Nkhani ya Yona—Yophunzitsa Kulimba Mtima Komanso Chifundo (Yona 1-4)
-
2:40 Nyimbo Na. 71 ndi Zilengezo
-
2:50 Amene Ali Kumbali Yathu ndi Ambiri Kuposa Amene Akutitsutsa (Deuteronomo 7:17, 21; 28:2; 2 Mafumu 6:16; 2 Mbiri 14:9-11; 32:7, 8, 21; Yesaya 41:10-13)
-
3:50 Nyimbo Yomaliza Komanso Pemphero