Kalozera wa Mafanizo
Manambalawa akusonyeza mutu umene fanizolo likupezeka
mbalame komanso maluwa 35
kumanga nsanja 84
ngamila ikhoza kulowa pa diso la singano 96
ana amene anakhala pansi mumsika 39
kusankha malo olemekezeka 83
alimi anapha mwana wa mwiniwake wa munda 106
aganyu anawapatsa ndalama ya dinari 97
ndalama ya dalakima inapezeka 85
khoka 43
kapolo wokhulupirira ndi wanzeru 111
woyang’anira nyumba wokhulupirika 78
bambo amafunitsitsa kupatsa ana ake zinthu zabwino 35
mtengo wa mkuyu 79
M’busa Wabwino 80
asodzi a anthu 22
maziko a nyumba 35
kambewu ka tirigu kamafa, kenako kamamera 103
nkhuku ya thadzi imasonkhanitsa ana ake 110
nyumba yomangidwa pathanthwe 35
kuitanira anthu osauka ku phwando 83
mfumu inakhululuka ngongole yaikulu 64
mfumu imene ikufuna kukamenya nkhondo 84
mfumu inakonza phwando la ukwati 107
ufa wosakaniza ndi zofufumitsa 43
zofufumitsa za Afarisi 58
ndalama ya dalakima imene inasowa 85
nkhosa yosochera 63
anthu anakana ataitanidwa 83
ndalama ya mina 100
alimi omwe anapha anthu 106
kambewu kampiru, chikhulupiriro 89
kambewu kampiru, Ufumu 43
chipata chopapatiza 35
diso la singano 96
Msamariya wachifundo 73
vinyo watsopano, matumba akale a vinyo 28
ngale ya mtengo wapatali 43
musamaponyere nkhumba ngale zanu 35
bwenzi lokakamira 74
mwana wotayika 86
wogwira pulawo 65
munthu wolemera komanso Lazaro 88
munthu wolemera yemwe anamanga nkhokwe zazikulu 77
mchere wa dziko 35
mbewu zinagwera panthaka yosiyanasiyana 43
kusokerera chigamba chatsopano pa nsalu yakale 28
nkhosa komanso mbuzi 114
kapolo amene akuchokera kumunda 89
akapolo amene ankayembekezera kubwera kwa mbuye wawo 78
mwana wotayika 86
wofesa mbewu 43
wofesa mbewu amene anagona 43
kusefa nyerere, kumeza ngamila 109
kachitsotso m’diso la m’bale wako 35
matalente 113
wokhometsa msonkho komanso Mfarisi 94
anamwali 10 112
chuma chomwe chinabisidwa m’munda 43
mtengo wa mpesa weniweni 120
ana awiri anatumidwa kuti apite kumunda wa mpesa 106
anthu awiri amene anabwereka ndalama 40
mizimu yonyansa inabwerera 42
kapolo wosakhululuka 64
woyang’anira nyumba wosalungama 87
tirigu ndi namsongole 43
mkazi wamasiye ndi woweruza 94
ogwira ntchito m’munda wa mpesa 97
KALOZERA WA MABOKOSI
‘Masiku Akuti Ayeretsedwe Anakwanira’ 6
Maulendo Osangalatsa 10
Kodi Asamariya Anachokera Kuti? 19
Munthu Wogwidwa Ndi Mzimu Woipa 23
Mafanizo Onena za Kusala Kudya 28
Ankabwereza Mfundo Pophunzitsa 35
Thukuta la Yesu Linaoneka Ngati Madontho a Magazi 123
Munda wa Magazi 127
Kukwapula 129
“M’pachikeni” 132