GAWO 2
Mmene Utumiki wa Yesu Unayambira
“Taonani, Mwanawankhosa wa Mulungu amene akuchotsa uchimo.”—Yohane 1:29
M'CHIGAWO ICHI
MUTU 12
Zimene Zinachitika Pamene Yesu Ankabatizidwa
Popeza Yesu analibe uchimo, n’chifukwa chiyani anabatizidwa?
MUTU 13
Zimene Yesu Anachita Atayesedwa
Zimene Yesu anakumana nazo poyesedwa zimatithandiza kudziwa mfundo ziwiri zokhudza Mdyerekezi.
MUTU 14
Yesu Anayamba Kupeza Ophunzira
N’chiyani chinatsimikizira ophunzira 6 oyambirira a Yesu kuti apeza Mesiya?
MUTU 15
Chozizwitsa Choyamba Chimene Yesu Anachita
Zimene Yesu anayankha mayi ake zinasonyeza kuti cholinga chake chinali kuchita zimene Atate wake wakumwamba amuuza, osati zimene mayi akewo anamuuza.
MUTU 16
Yesu Anali Wodzipereka pa Kulambira Mulungu
Chilamulo cha Mulungu chinkalola anthu kugula nyama zoti apereke nsembe ku Yerusalemu, nanga n’chifukwa chiyani Yesu anakwiya ndi amalonda mu kachisi?
MUTU 18
Ntchito ya Yesu Inayamba Kuwonjezeka Kuposa ya Yohane
Ophunzira a Yohane M’batizi ankachita nsanje ngakhale kuti Yohane sankachita nsanje.
MUTU 19
Yesu Analalikira Mayi wa ku Samariya
Yesu anamuuza zinthu zimene anali asanauzepo munthu aliyense.