Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

GAWO 2

Mmene Utumiki wa Yesu Unayambira

“Taonani, Mwanawankhosa wa Mulungu amene akuchotsa uchimo.”—Yohane 1:29

Mmene Utumiki wa Yesu Unayambira

M'CHIGAWO ICHI

MUTU 12

Zimene Zinachitika Pamene Yesu Ankabatizidwa

Popeza Yesu analibe uchimo, n’chifukwa chiyani anabatizidwa?

MUTU 13

Zimene Yesu Anachita Atayesedwa

Zimene Yesu anakumana nazo poyesedwa zimatithandiza kudziwa mfundo ziwiri zokhudza Mdyerekezi.

MUTU 14

Yesu Anayamba Kupeza Ophunzira

N’chiyani chinatsimikizira ophunzira 6 oyambirira a Yesu kuti apeza Mesiya?

MUTU 15

Chozizwitsa Choyamba Chimene Yesu Anachita

Zimene Yesu anayankha mayi ake zinasonyeza kuti cholinga chake chinali kuchita zimene Atate wake wakumwamba amuuza, osati zimene mayi akewo anamuuza.

MUTU 16

Yesu Anali Wodzipereka pa Kulambira Mulungu

Chilamulo cha Mulungu chinkalola anthu kugula nyama zoti apereke nsembe ku Yerusalemu, nanga n’chifukwa chiyani Yesu anakwiya ndi amalonda mu kachisi?

MUTU 17

Yesu Anaphunzitsa Nikodemo

Kodi “kubadwanso” kumatanthauza chiyani?

MUTU 18

Ntchito ya Yesu Inayamba Kuwonjezeka Kuposa ya Yohane

Ophunzira a Yohane M’batizi ankachita nsanje ngakhale kuti Yohane sankachita nsanje.

MUTU 19

Yesu Analalikira Mayi wa ku Samariya

Yesu anamuuza zinthu zimene anali asanauzepo munthu aliyense.