Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

January 8, 2001

Kodi Ukwati Wathu Tingaupulumutse?

Kodi kukhala mu ukwati wopanda chikondi ndiko njira yabwinopo poyerekeza ndi kusudzulana? Kodi mwamuna ndi mkazi amene chikondi chawo chazirala angapulumutse motani ukwati wawo?

3 Zikuvuta Kuchoka mu Ukwati Wopanda Chikondi

4 N’chifukwa Chiyani Chikondi Chimazirala?

7 Kodi Pali Chifukwa Chokhalira ndi Chiyembekezo?

8 Ukwati Wanuwo Utha Kupulumuka!

15 Inali Yoyamba Zaka 100 Zapitazo

18 Achinyamata Akufunsa Kuti

Kodi Tsopano Ndikhala Bwanji Pamene Abambo Atichokera?

21 Kodi N’kuti Kumene Mungapeze Maphunziro Abwino Kwambiri?

22 Ntchito Yamaphunziro Yofala Kwambiri

30 Lingaliro la Baibulo

Kusankha Chithandizo cha Mankhwala—Kodi N’kofunikira?

32 Sakhulupirira Kwenikweni Koma Akufufuzabe

Maphunziro Othandiza kwa Moyo Wonse 28

Ŵerengani za ndawala yophunzitsa imene imagogomezera miyezo yapamwamba yamakhalidwe, yopereka moyo wabwinopo, ndiponso yopereka chiyembekezo cholimba cha m’tsogolo.