Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zisonyezero za Voliyumu 83 ya Galamukani!

Zisonyezero za Voliyumu 83 ya Galamukani!

Zisonyezero za Voliyumu 83 ya Galamukani!

ACHINYAMATA AKUFUNSA

Anthu Okhala M’chipinda Chimodzi, 5/8, 6/8, 7/8

Khalidwe la Anzanga, 12/8,

Kodi Mukufunika Telefoni ya M’manja? 11/8

Kodi N’Chifukwa Chiyani Kholo Langa Silindikonda? 10/8

Kodi Pali Vuto Lotani Ndi Zamatsenga? 2/8

Kukhala N’chibwenzi, 1/8

Kukhala Wokongola, 8/8

Kulalikira Anzanu Akusukulu? 3/8, 4/8

Opaleshoni Yodzikongoletsa, 9/8

CHIPEMBEDZO

Kodi Mdyerekezi Alikodi? 3/8

“Kupemphera Pawekha,” 5/8

Mapemphero Opempha Mtendere, 11/8

CHUMA NDI NTCHITO

Aphunzitsi, 3/8

Kumalo Antchito Nkotetezeka Bwanji? 3/8

Malingaliro Oyenera a Ntchito, 3/8

LINGALIRO LA BAIBULO

Chikondwerero cha Chaka Chatsopano, 1/8

Khirisimasi, 12/8

Kodi Akristu Ayenera Kulalikira? 6/8

Kodi Mulungu Amanyalanyaza Zofooka? 11/8

Kodi Mulungu Amavomereza Nkhondo? 5/8

Kudziona Ngati Wolakwa, 3/8

Kutetezedwa ndi Mulungu, 4/8

Maphempero Amene Mulungu Amamva, 9/8

Mikaeli Mngelo Wamkulu, 2/8

Mmene Mulungu Amachionera Chiwawa, 8/8

Zinthu Zakale Zofukulidwa Pansi, 10/8

Zithunzi Zolaula, 7/8

MAUNANSI A ANTHU

Amayi, 4/8

Kulimbikitsa Amene Akulira Maliro, 5/8

Mabanja Akholo Limodzi, 10/8

Tsiku Laukwati, 2/8

Ukwati Ndiwo Mgwirizano Wosatha, 2/8

MAYIKO NDI ANTHU

Amasai—Anthu Odabwitsa Ndiponso Ochititsa Kaso, 3/8

Kupulumuka Zoopsa Phiri Litaphulika N’kumatuluka Chiphalaphala (Congo [Kinshasa]), 11/8

MBONI ZA YEHOVA

Kugwiritsa Ntchito Galamukani! Mwanjira Yabwino, 9/8

Kuthandiza Anthu Amene Tsoka Lalikulu Linawagwera (Texas, U.S.A.), 12/8

Kutsutsana Pankhani Anaonetsa pa TV (Georgia), 8/8

Misonkhano Yachigawo ya “Olengeza Ufumu Achangu,” 6/8

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Kudalira Mulungu Kunandilimbitsa (R. Sacksioni-Levee), 1/8

Kukumananso Modabwitsa (D. Sheets, M. Ruge), 11/8

Wandale Anasanduka Mkristu Wosakhudzidwa N’zandale (L. Šmejkal), 7/8

SAYANSI

Kodi Sayansi ndi Chipembedzo Zingagwirizane? 6/8

Mdima Ukagwa Masana (Kadamsana), 9/8

UMOYO NDI MANKHWALA

Achinyamata Ovutika ndi Tulo, 8/8

Chakudya Chopatsa Thanzi, 5/8

Chakudya Chosakayikitsa, 1/8

Dzitetezeni Kuti Musagonthe M’kutu! 6/8

Edzi, 11/8

Matenda a Kuthamanga kwa Magazi, 5/8

Ndinapita Padera, 4/8

Uchi—Mankhwala Ozuna, 3/8

Vuto la Kusokonezeka Maganizo Atabereka, 8/8

ZINYAMA NDI ZOMERA

Chakumwa Chochokera ku Chitsamba Chachilendo, 5/8

Chinenero cha Kutchire—Kulankhulana kwa Zinyama, 4/8

Mbidzi, 2/8

Tizilombo Tochotsa Nyansi, 6/8

ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE

Kodi Apolisi Ndi Ofunika Chifukwa Chiyani? 7/8

Kodi Kuyenda Pandege N’kwabwinobe? 12/8

Kodi Nzongopeka Kuti Dziko Lonse Lidzakhala Pamtendere? 5/8

Kudalirana kwa Mayiko, 6/8

Kuphunzirapo Kanthu Pazochitika Zakumbuyoku, 8/8

Kutchova Njuga, 8/8

Mabanja Akholo Limodzi, 10/8

Opulumuka Chivomezi, 4/8

Othawa Kwawo, 2/8

Tsiku Limene Nyumba Zosanja Ziŵiri Zinagwa, 1/8

Ukapolo, 7/8

Zida Zofalitsa Tizilombo Topereka Matenda, 10/8

Zinyalala, 9/8

ZOSIYANASIYANA

Anthu Okonda Zinthu Zonyamula Mtima, 10/8

Kodi Anali Munthu Wolimbikitsa Nkhondo? (Alfred B. Nobel), 5/8

Manambala (Zokhulupirira Manambala), 9/8

Ngozi Zapamsewu, 9/8

Zombo Zamphamvu (zoswa ayezi), 12/8