Zamkatimu
Zamkatimu
April 8, 2003
Mungatani Ngati Mwana Wanu Anayamba Mankhwala Osokoneza Bongo?
Achinyamata ambiri padziko lonse ayamba mankhwala osokoneza bongo. Kodi makolo angawathandize motani ana awo?
3 Mankhwala Osokoneza Bongo Pakati pa Achinyamata
10 Vuto la Mankhwalaŵa Litha Posachedwapa Padziko Lonse
11 Kodi Kugona N’kofunikadi Kapena Sikofunika Kwenikweni?
14 Zimene Mungachite Kuti Muzigona Bwino
23 Kudya Opanda Mafoloko ndi Mipeni
26 Ulendo Wokaona Munda wa Nthochi
29 Miyambi ya Aakani Imasonyeza Chikhalidwe Chawo
32 Msonkhano Wofunika Kwambiri Pachaka
Kodi Kukonda Chuma N’kutani Makamaka? 18
Kodi Baibulo limatipo chiyani pankhani ya kukhala ndi chuma?
Kodi Ndizisankha Motani Matepi a Nyimbo Oti Ndizionera? 20
Achinyamata ambiri amakonda kuonera matepi a nyimbo. Kodi ndi mfundo za m’Baibulo ziti zimene zingakuthandizeni kusankha nyimbo zabwino zoti muzionera?