Zamkatimu
Zamkatimu
January 8, 2004
Kumvetsetsa Matenda A Maganizo
Padziko lonse, matenda a maganizo ochititsa munthu kungokhala woipidwa ndiponso ochititsa munthu kusinthasintha zochitika amasautsa amuna ndi akazi ambimbiri. Kodi odwala matendaŵa angathandizidwe bwanji?
4 Kukhala ndi Matenda a Maganizo
8 Nkhani Yabwino kwa Odwala Matendaŵa
16 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .
Kodi Ndingathe Bwanji Kukamba Nkhani Bwino Pagulu?
19 Kubadwira M’dziko Lopanda Chikondi!
20 Zimene Makanda Amafunikira Ndiponso Zimene Amafuna
24 Kupatsa Ana Zimene Amafunikira
31 Zomera N’zothandiza Kwambiri Popanga Mankhwala
32 Kukhalabe Osangalala Ngakhale M’mavuto
Kodi Zokambirana za Mayiko Zidzabweretsa Mtendere Padziko Lonse? 14
N’chifukwa chiyani anthu akamayesa kukambirana zamtendere kaŵirikaŵiri siziphula kanthu?
Kodi Mankhwala Ochokera ku Zitsamba Angakuthandizeni? 28
Mankhwala ochokera ku zitsamba ayamba kutchuka kwambiri. Koma kodi ndi zinthu zotani zimene n’kwanzeru kusamala nazo?