Zamkatimu
Zamkatimu
June 8, 2004
Kukhala Nokhanokha Koma Osasungulumwa
N’chifukwa chiyani anthu ambiri ali osungulumwa? Kodi munthu angachite chiyani kuti athane ndi kusungulumwa? Kodi padzakhala nthaŵi imene sipadzakhalanso munthu wosungulumwa?
3 N’chifukwa Chiyani Anthu Ambiri Ali Osungulumwa?
9 Nthaŵi Imene Sipadzakhalanso Munthu Wosungulumwa
18 N’chifukwa Chiyani Anthu Ambiri Amadwala Chimfine Chimene Chimabwera Akakhala Pafupi ndi Mungu?
19 Nkhondo Yakalekale Yofuna Kupeza Thanzi Labwino
23 Kupambana ndi Kulephera pa Nkhondo Yolimbana ndi Matenda
30 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .
N’chifukwa Chiyani Chibwenzi Changa Chimandizunza Chonchi?
Matayala Angapulumutse Moyo Wanu 12
Matayala abwino ndi ofunika kwambiri kuti galimoto isachite ngozi. Kodi mungawasamale bwanji?
Kodi Kuda Nkhaŵa N’kupanda Chikhulupiriro? 16
Kodi Baibulo limati chiyani pa nkhani imeneyi?