Zamkatimu
Zamkatimu
October 8, 2004
Vuto Lapadziko Lonse la Atsikana Otenga Mimba Ali Aang’ono
Atsikana ambiri amakhala ndi vuto lolera okha ana. Kodi zingatheke kuti zinthu ziwayendere bwino? Kodi njira yabwino kwambiri yothandizira atsikana kuti apeŵe vuto limeneli ndi yotani?
3 Kusanduka Azimayi Akadali Ana
4 Vuto Lapadziko Lonse la Atsikana Otenga Mimba Ali Aang’ono
8 Kulimbana ndi Mavuto Amene Amakhalapo Munthu Akakhala Mayi Akadali Wamng’ono
11 Kuthandiza ndi Kuteteza Atsikana
18 Sukulu Yamkaka Yopanda Zoseŵeretsa
19 Ana Ambiri Akubadwa Kudzera M’njira Zothandizira Anthu Osabereka Kuti Abereke
22 Njira Zatsopanozi Zabweretsanso Mavuto Atsopano
22 Matenda Osintha Mtundu wa Khungu
32 Izi N’zomwe Achinyamata Amafunikira
Kodi Anthu Okalamba Tiyenera Kuwachitira Zinthu Motani? 16
Malipoti akusonyeza kuti m’mayiko ambiri, anthu okalamba akunyalanyazidwa ndi kuchitiridwa nkhanza. Kodi Baibulo limaphunzitsa kuti okalamba tiziwaona bwanji?
Kodi Kumwa Moŵa Wambiri Nthaŵi Imodzi Kuli ndi Vuto Lanji? 29
Kodi kumwa moŵa wambiri nthaŵi imodzi n’kutani? Kodi kuopsa komwa moŵa mwauchidakwa n’kotani, makamaka kwa achinyamata?