Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

November 8, 2004

Kodi Makolo Ayenera Kuchita Chiyani pa Zaka Zoyambirira za Moyo wa Mwana Wawo?

Makolo amafuna kuti ana awo akule bwino n’kudzakhala achikulire oti zinthu zidzawayendere bwino. Kodi angachite chiyani kuti zimenezi zidzachitikedi? Kodi njira yabwino kwambiri yolimbikitsira mwana wanu kuchita zonse zomwe angathe ndi yotani?

3 Kodi Kuphunzitsa Mwana Kuyambira Ali Wakhanda N’kofunika Motani?

5 Kufunika Kolimbikitsa Mwana Wanu Kuphunzira

7 Udindo Wanu Monga Kholo

11 Kodi Kunenepa Kwambiri Ndi Vutodi?

12 Kodi N’chiyani Chimachititsa Anthu Kunenepa Kwambiri?

15 Kodi Kunenepa Kwambiri Mungakuthetse Bwanji?

18 Kodi Kuchita Khama Kuti Muchepetse Kunenepa N’kwaphindudi?

21 Ndinaphunzitsidwa Kukonda Mulungu Kuyambira Ndili Mwana

28 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .

Kodi Mnyamata Ndingamuuze Bwanji Kuti Ndikumufuna?

31 Ubwino Woŵerengera Ana

32 Angatonthoze Anamalira

Kulera Ana M’maleredwe a Mulungu 26

Kodi mfundo za m’Baibulo zingathandize bwanji makolo kuphunzitsa ana awo?