Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

February 8, 2005

Zimene Mungachite Kuti Moyo Wanu Usakhale Wopanikizika

Akatswiri ambiri akukhulupirira kuti kukhala ndi moyo wopanikizika kungawononge kwambiri thanzi la munthu. Kodi zinthu zina zimene zimachititsa moyo kukhala wopanikizika masiku ano n’ziti? Werengani nkhani zofotokoza zinthu zina zomwe mungachite kuti muchepetse kupanikizika pamoyo wanu.

3 Kusowa Mtendere Chifukwa cha Moyo Wopanikizika

4 Zimene Zimachititsa Moyo Kukhala Wopanikizika ndi Zotsatirapo Zake

7 Pali Zimene Mungachite Kuti Moyo Wanu Usakhale Wopanikizika

17 Zimene Zikuchitikira Madokotala M’dziko Limene Likusinthali

19 Madokotala Amakumana N’zambiri

22 Kodi Udokotala uli ndi Tsogolo Lotani?

26 Kodi Mafoni A M’manja ndi Abwino Kapena ndi Oipa?

29 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .

Kodi Ndiyenera Kutani Anthu Ena Akandiuza Mavuto Awo?

32 Buku la Achinyamata Limene Ambiri Amaliyamikira

Kupatsa Ana Chisamaliro Chimene Amafunikira 12

Kodi makolo ayenera kuchita chiyani kuti apatse ana awo chisamaliro chimene amafunikira?

“Ndinu Dr. Livingstone, Eti?” 14

Kukumana kwa Stanley ndi Livingstone kunali kochititsa chidwi kwambiri, komanso kunali kothandiza m’njira zina. Onani zifukwa zomwe ntchito ya amuna awiri amenewa yakhudzira kwambiri miyoyo ya anthu ochuluka.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

From the book Missionary Travels and Researches in South Africa, 1858