Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mlozera Nkhani wa Voliyumu 86 ya Galamukani!

Mlozera Nkhani wa Voliyumu 86 ya Galamukani!

Mlozera Nkhani wa Voliyumu 86 ya Galamukani!

ACHINYAMATA AKUFUNSA

Anthu Ena Akandiuza Mavuto Awo, 2/8

Kucheza ndi Anthu Olakwika, 8/8, 9/8

Kucheza ndi Anthu pa Intaneti, 10/8, 11/8

Kupeza Chibwenzi pa Intaneti, 5/8, 6/8

Ndingatani Kuti Ndiziugwira Mtima? 3/8

Ndingatani Mnyamata Amene Ndimamufuna Akandikana? 1/8

Ndingatani Ngati Mtsikana Akundifuna? 7/8

Ndizigwira Ntchito Yamanja Chifukwa Chiyani? 4/8

Tichite Kukhala ndi Mwambo Wonse wa Ukwati? 12/8

CHIPEMBEDZO

Kodi Yesu Kristu Ndi Mulungu? 5/8

CHUMA NDI NTCHITO

Kupeza ndi Kukhalitsa Pantchito, 7/8

MAUNANSI A ANTHU

Amayi Ndi Aphunzitsi, 3/8

Kukongola Kofunika Kwambiri, 1/8

Kumvetsa Mavuto Amene Dokotala Wanu Akukumana Nawo, 2/8

Kuthandiza Achinyamata Amene Ali Pamavuto, 4/8

MAYIKO NDI ANTHU

Chigwa cha Ngorongoro (Tanzania), 1/8

Malo Ovuta Kuwamvetsa a ku Africa, 11/08

“Ndinu Dr. Livingstone, Eti?” (Tanzania), 2/8

Nyanja ya Pinki (Senegal), 10/8

“Palibe Mawu Otukwana” (mtundu wa Apache), 7/8

“Tikakumane Pachitsime” (Moldova), 11/8

MBONI ZA YEHOVA

Achinyamata Amalalikira Mogwira Mtima, 9/8

Kupereka Umboni Wabwino ku Sukulu (Mexico), 10/8

Kusintha Akaidi, 4/8

Mulungu Amalemekezeka Tikamachita Zinthu Moona Mtima, 9/8

“Muzinyadira Zimenezi,” 6/8

Ndende za ku Mexico, 10/8

“Ndikanakonda Anthu Akanadziwa Zimenezi!” (Dominican Republic), 1/8

Nkhani Yakale Inakhudza Mitima ya Anthu, 8/8

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Kukopeka ndi Mlengi Chifukwa cha Kukongola kwa Choonadi (T. Fujii), 8/8

Kwalembedwa Kuti Ndidzawaonanso (R. Phillips), 1/8

Ndinafunitsitsa Kukwanitsa Cholinga Changa (M. Serna), 7/8

Ndinatha Kutumikira Mulungu Ngakhale Zinali Zovuta (I. Mikitkov), 5/8

Nkhondo Imene Inasintha Moyo Wanga (M. Molina), 11/8

Sayansi ndi Baibulo Zinandithandiza Kudziwa Cholinga cha Moyo (B. Oelschlägel), 12/8

Tinapeza Chinachake Chabwino Koposa (F. Del Rosario de Páez), 9/8

Wokonzeka Kuthandiza Ena (C. Vavy), 3/8

Zilema Zanga Sizinandifooketse (K. N’Guessan), 12/8

SAYANSI

Dzuwa Kuwala Pakati pa Usiku, 6/8

UMOYO NDI MANKHWALA

Khansa Yapakhungu, 6/8

Kuchita Zinthu Zolimbitsa Thupi, 6/8

Kumvetsa Mavuto Amene Dokotala Wanu Akukumana Nawo, 2/8

Kumwa Mowa Mopitirira Muyeso, 10/8

Moyo Wopanikizika, 2/8

Utsi Wakupha (wa nkhuni), 6/8

ZIMENE BAIBULO LIMANENA

Kodi Akazi Azibisa Kukongola Kwawo? 10/8

Kodi Baibulo Limapondereza Akazi? 11/8

Kodi Kufatsa N’kupanda Mphamvu? 1/8

Kodi Kufuna Kutchuka N’kulakwa? 6/8

Kodi Mulungu Ali Paliponse? 3/8

Kodi Mulungu Amakondera Mitundu Ina ya Anthu? 12/8

Kodi Muyenera Kuopa Armagedo? 7/8

Kodi Nyenyezi Zingakuthandizeni Kudziwa Tsogolo Lanu? 8/8

Kugwiritsa Ntchito Zithunzi Popemphera, 5/8

Kupatsa Ana Chisamaliro Chimene Amafunikira, 2/8

Kupemphera kwa Mariya Virigo? 9/8

Maukwati a Amuna Okhaokha Kapena Akazi Okhaokha, 4/8

ZINYAMA NDI ZOMERA

Mgwirizano, 9/8

Tomato, 3/8

ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE

Dziko Likusakazidwa Kwabasi, 1/8

Kuba M’masitolo, 7/8

Kudyetsa Anthu Wani Biliyoni, 8/8

Kukhala Mopanda Mantha, 8/8

Kupezera Chakudya Anthu Okhala M’mizinda, 12/8

Kusowa Pokhala, 12/8

Mafilimu, 5/8

Masoka Achilengedwe, 8/8

Mmene Mungapindulire ndi Manyuzipepala, 11/8

Msampha wa Kumwa Mowa Mopitirira Muyeso, 10/8

Njira Zosawononga Dziko Zopangira Magetsi, 3/8

Ntchito Zokopa Alendo, 9/8

Vuto la Padziko Lonse la Kusowa kwa Nyumba, 10/8

Zimene Osauka Angayembekezere, 11/8

ZOSIYANASIYANA

Mafoni a M’manja Ndi Abwino Kapena Ndi Oipa? 2/8

Mapiri Ndi Ofunika kwa Zamoyo, 4/8

Mumayendetsa Galimoto Mbali Iti ya Msewu? 4/8

Pakhomo Paukhondo, 6/8