Zamkatimu
Zamkatimu
February 2006
Kupirira Mavuto a Ukalamba
Kodi munthu angapirire bwanji mavuto a ukalamba? Mu nkhani zimenezi muli malangizo amene angathandize munthu kusangalalako ndi ukalamba.
3 Kodi Ukalamba Ungakhaledi Wosangalatsa?
8 Kukhala ndi Mphamvu Ngati Wachinyamata Mpaka Muyaya
10 Kodi Angelezi Oyambirira Kusamukira ku America Anali Akristu Oona?
18 Zimene Achinyamata Amadzifunsa
Kodi Ndingatani Kuti Ndisiye Kudzivulaza?
21 Kukaona Malo Opangira Ziwalo
24 Mtsinje wa Thames Wachita Zazikulu M’mbiri ya England
Alhambra—Nyumba Yachisilamu Yokongola Kwambiri ya ku Granada 14
Anthu ambirimbiri apitako kukaona nyumba yomangidwa mwachisilamu yochititsa chidwi imeneyi, ndipo agoma poona momwe madzi anagwiritsiridwa ntchito pa nyumbayi.
Kodi Pali Mulungu Mmodzi Yekha Woona? 28
Pali milungu yambiri imene anthu amalambira, koma kodi pali Mulungu mmodzi woona? Tikudziwa bwanji zimenezi?
[Mawu a Chithunzi patsamba 2]
J. A. Fernández/San Marcos