Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

February 2006

Kupirira Mavuto a Ukalamba

Kodi munthu angapirire bwanji mavuto a ukalamba? Mu nkhani zimenezi muli malangizo amene angathandize munthu kusangalalako ndi ukalamba.

3 Kodi Ukalamba Ungakhaledi Wosangalatsa?

4 Kupirira Mavuto a Ukalamba

8 Kukhala ndi Mphamvu Ngati Wachinyamata Mpaka Muyaya

10 Kodi Angelezi Oyambirira Kusamukira ku America Anali Akristu Oona?

18 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndingatani Kuti Ndisiye Kudzivulaza?

21 Kukaona Malo Opangira Ziwalo

24 Mtsinje wa Thames Wachita Zazikulu M’mbiri ya England

30 Zochitika Padzikoli

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 “N’kabwino Kwabasi!”

Alhambra—Nyumba Yachisilamu Yokongola Kwambiri ya ku Granada 14

Anthu ambirimbiri apitako kukaona nyumba yomangidwa mwachisilamu yochititsa chidwi imeneyi, ndipo agoma poona momwe madzi anagwiritsiridwa ntchito pa nyumbayi.

Kodi Pali Mulungu Mmodzi Yekha Woona? 28

Pali milungu yambiri imene anthu amalambira, koma kodi pali Mulungu mmodzi woona? Tikudziwa bwanji zimenezi?

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

J. A. Fernández/San Marcos