Zamkatimu
Zamkatimu
March 2006
Kodi Chikondi Chapita Kuti?
Masiku ano, anthu ambiri amaona kuti sakondedwa. Komabe, chikondi n’chofunika kwambiri kuti tizisangalala ndiponso kuti tizikhala ndi moyo wabwino. Phunzirani mmene mungakhalire ndi khalidwe lapadera limeneli.
4 Chifukwa Chake Chikondi Chenicheni N’chovuta Kupeza
8 Mmene Mungapezere Chikondi Chenicheni
10 Kulandira Mafoni Angozi ku London
Kodi Yesu Analidi Mwana wa Mulungu?
18 Nthanga Imene Inazungulira Dziko
24 Ulendo Wokaona Nkhosa Zam’tchire
26 Zimene Achinyamata Amadzifunsa
Kodi Ndingapewe Bwanji Zogonana Kusukulu?
32 Tsiku Lofunika Kwambiri M’mbiri Yonse ya Anthu
Chilumba Chokongola Kwambiri cha Mchenga 14
Bwerani nafe pamene tikupita kukaona chilumba chokongola ku dera lofunda kum’mwera kwa matanthwe a m’nyanja opangidwa ndi zamoyo zing’onozing’ono otchedwa Great Barrier Reef ku Australia
‘Ndikufuna Kutumikira Mulungu Ndisanafe’ 21
Pamene Mamie anali ndi zaka 12, anathawa kwawo nyumba yawo ikuyaka moto pankhondo yapachiweniweni. Anawombedwa ndi chipolopolo ndipo anthu ankaganiza kuti amwalira. Werengani nkhani yake yokhudza mtima.
[Mawu a Chithunzi patsamba 2]
Courtesy of Tourism Queensland