Zamkatimu
Zamkatimu
April 2006
Mungachipeze Bwanji?
Anthu ambiri amayesetsa kuti apeze chimwemwe, koma zimaoneka kuti ndi ochepa amene amachipeza. Chifukwa chiyani? Kodi chinsinsi chopezera chimwemwe chagona pati?
3 Mungathe Kupeza Chimwemwe Chenicheni
4 Njira Yopezera Chimwemwe Chenicheni
10 “Anaikidwa M’ndende Chifukwa cha Chikhulupiriro Chawo”
17 Zimene Achinyamata Amadzifunsa
Kodi Kucheza ndi Anzanga a Ku Sukulu Kumapyola Malire Kukafika Pati?
20 Ndinaphunzira Kudalira Mulungu
Ulendo wa Tsiku Limodzi wa ku Chernobyl 14
April ndi mwezi wokumbukira kuti patha zaka 20 chichitikireni ngozi yoopsa kwambiri ya nyukiliya yomwe inachitika panthawi yoti si yankhondo. Kodi anthu akupirira bwanji zotsatira za ngozi imeneyi?
Kulera Ana Omwe Amafunika Kuwamasalira Mwapadera 25
Anthu okwana atatu pa anthu 100 alionse padziko lapansi pano akuti ali ndi vuto linalake loganiza moperewera. Onani momwe mabanja akupiririra bwinobwino ngakhale kuti ali ndi ana amene ali ndi mavutowa.