Zamkatimu
Zamkatimu
June 2006
Uchigawenga Ukadzatha
Uchigawenga wakhalapo kwa zaka zambiri, koma masiku ano umavutitsa anthu ambiri kuposa kale lonse. Kodi udzatha liti, ndipo udzatha bwanji?
3 Ana Akuvutika ndi Uchigawenga
4 Mbiri Yodzaza ndi Kukhetsa Magazi
7 Mtendere Udzabweradi Padziko Lapansi!
20 Mmene Kujambula Zithunzi Kunayambira
24 Silika—“Nsalu Yapamwamba Kwambiri”
Kodi Tchimo Loyambirira Linali Chiyani?
32 Anthu Ambiri Adzapita Kodi Inunso Mudzapita Nawo?
Kodi Ndingatani Kuti Ndizisamala Ndalama? 10
Kuwononga ndalama n’kosavuta. Kodi chinsinsi chopangira bajeti yabwino n’chiyani?
Kumvera Machenjezo Kunawathandiza 14
Kodi pakuchitika zotani pothandiza anthu amene anakhudzidwa ndi mphepo za mkuntho za Katrina ndi Rita?
[Mawu a Chithunzi patsamba 2]
AP Photo/Ben Sklar