Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

July 2006

Mmene Mungakhalire ndi Banja Losanga lala

Masiku ano pali zinthu zambiri zimene zikutekesa mabanja. Onani mmene mungalimbitsire banja lanu potsatira mfundo zabwino komanso zothandiza kuti banja lonse likhale losangalala.

3 Kodi Banja Lingapirire Mavuto Aakulu?

6 Mmene Mungakhalire ndi Banja Losangalala

10 Uthenga Uyenera Kuperekedwa

14 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Mzimu Woyera Ndi Munthu?

16 N’chifukwa Chiyani Madzi a M’nyanja Zikuluzikulu Amakhala Amchere?

19 Nsomba Zikakudwalitsani

22 Kodi Kusisita Mwana N’kofunika?

23 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndidzagwire Ntchito Yotani Pamoyo Wanga?

29 Zochitika Padzikoli

30 Kuchokera kwa Owerenga

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Kodi N’zotheka Kuti Banja Likhale Losangalala?

Ndinali Wotaya Mtima Koma Tsopano Ndine Wosangalala 11

Mnyamata wina anakonza zodzipha chifukwa chodziimba mlandu ndiponso kuthedwa nzeru. Imvani mmene Mawu a Mulungu anam’thandizira kukhala ndi mtendere weniweni wa mumtima.

‘Katswiri wa ku Britain Yemwe Anaiwalika’ 26

Katswiriyu anali ndi moyo m’nthawi ya Isaac Newton, ndipo anali mmodzi mwa akatswiri a ku Britain amene anatulukira kapangidwe ka zinthu zosiyanasiyana. Koma m’mbuyomu sanali kutchulidwa kawirikawiri m’mabuku a mbiri yakale. Onani zomwe zinachititsa.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Images courtesy of the Posner Memorial Collection, Carnegie Mellon University Libraries