Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

April 2007

N’chifukwa Chiyani Makhalidwe Alowa Pansi?

Padziko lonse makhalidwe alowa pansi kwambiri. Kodi zimenezi kwenikweni zinayamba liti ndipo n’chifukwa chiyani zinachitika nthawi imeneyo? Kodi dziko lathu likulowera kuti?

3 Makhalidwe Akulowa Pansi Padziko Lonse

4 Nthawi Imene Makhalidwe Analowa Pansi Kwambiri

8 Kodi Dzikoli Likulowera Kuti?

14 Kuchoka ku Iguputo Kupita ku Mizindayambiripadzikoli

19 Chinthu Chokhalitsa Kuposa Luso la Zosemasema ndi Zoumbaumba

23 Thanthwe Lochititsa Chidwi

24 Kunika Nsalu Kwakale ndi Kwamasiku Ano

26 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Kukhala Mkhristu Kumatanthauza Chiyani?

28 Bwanji Ndimakomokakomoka?

29 Kuchokera kwa Owerenga

30 Zochitika Padzikoli

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 “Buku Labwino Kwambiri Pophunzitsa”

N’chifukwa Chiyani Anthu Amakonda Kundifananitsa ndi Ena? 11

Kodi n’chifukwa chiyani kufananitsidwa ndi anthu ena kumapweteka kwambiri? Kodi munthu angapindulepo chilichonse?

Mungu N’ngofunika Kwambiri Pamoyo 16

Kodi mungu n’chiyani makamaka? Nanga umathandiza bwanji pamoyo?