Zamkatimu
Zamkatimu
January 2008
Kodi Baibulo Limati Chiyani Pamchitidwe Wochitira Nkhanza Akazi?
Padziko lonse akazi akuchitiridwa nkhanza ndiponso kuponderezedwa. Moti zipembedzo zina zafika poyamba kulekerera mchitidwewu. Kodi Baibulo limati chiyani pankhaniyi?
3 Kuchitira Nkhanza Akazi Ndi Vuto la Padziko Lonse
4 Kodi Mulungu ndi Khristu Amaona Akazi Motani?
11 Kamudzi ka Asodzi Kanasintha N’kukhala Mzinda Waukulu
15 Nyama Zakuthengo Zimasangalala ku Gabon
22 Mlatho Umene Unali Kumangidwa Mobwerezabwereza
24 Kangaude
25 Nyanja Yapadera Koma Yakufa
Kodi Kukhala Mutu Wabanja Kumatanthauza Chiyani Kwenikweni?
32 Amalikonda Kuposa Chidole Chilichonse
Tiyeni tipitire limodzi ku Salzburg, m’dziko la Austria, kuti tikaone zidole zochita zisudzo.
Kodi Ndizichita Masewera a Pakompyuta? 18
Masewera ambiri a pakompyuta amakhala achiwawa komanso a zachiwerewere. Kodi Mkhristu angasankhe bwanji masewera oyenerera? Nanga kodi ayenera kuwononga nthawi yaitali motani akuchita masewerawa? Kodi pali masewera ena amene angachite?
[Mawu a Chithunzi patsamba 2]
By courtesy of the Salzburg Marionette Theatre