Zamkatimu
Zamkatimu
February 2008
Kodi Zachiwawa Zidzatha?
Anthu ambiri amangokhala mwamantha chifukwa cha zachiwawa zimene zikuchitika. Kodi pali njira iliyonse yothetsera zachiwawa zomwe zafala masiku anozi? Kapena tingoiwalako zoti vutoli lidzatha? Werengani zinthu zolimbikitsa zimene Baibulo limanena pankhaniyi.
3 Kodi Zachiwawa Zafika Poipa Zedi?
4 Kodi Zachiwawa Zingathetsedwe?
8 Posachedwapa Zachiwawa ‘Zidzatha’
Kodi Mulungu Amakhululuka Machimo Akuluakulu?
12 Ndinali Mkulu wa Asilikali Koma Tsopano Ndine “Msilikali wa Khristu”
19 Kodi Mipukutu Yakale Inalembedwa Liti?
Kukhala Bwinobwino M’chipale Chofewa 16
Madera akumidzi okutidwa ndi chipale chofewa amaoneka ngati alibe zamoyo zilizonse. Komatu si choncho ayi.
Kodi Ndingatani Ngati Ndili ndi Matenda Aakulu Kapena Chilema? 26
Onani mmene achinyamata anayi akupiririra matenda aakulu ndiponso kulemala.
[Mawu a Chithunzi patsamba 2]
Petrels: By courtesy of John R. Peiniger
[Mawu a Chithunzi patsamba 3]
Robson Fernandes/Agencia Estado/WpN