Zamkatimu
Zamkatimu
April 2008
Kodi Tili M’masiku Otsiriza?
Kodi mawu a m’Baibulo akuti “masiku otsiriza” amatanthauza chiyani? Kodi mawuwa amam’khudza bwanji munthu aliyense? Kodi zinthu zidzakhala bwino m’tsogolo?
3 Kodi Ndi Masiku Otsiriza a Chiyani?
4 Kodi Masiku Otsiriza Ndi Ati?
8 Masiku Otsiriza Akadzatha Zinthu Zidzakhala Bwanji?
16 Mafuta a Golide a ku Mediterranean
Kodi Mulungu Amafuna Kuti Muzichita Chiyani?
32 Mmene Achinyamata Angathetsere Kuvutika Maganizo
Oona za Ndege Amakutetezani Bwanji? 13
Nthawi iliyonse ndege zambirimbiri zimakhala zikuuluka, ndiye kodi oona za kayendedwe ka ndege amathandiza bwanji kuti ndegezi zisagundane? Kodi mumakhaladi otetezeka mukakwera ndege?
N’chifukwa Chiyani Makolo Anga Sandikhulupirira? 27
Kodi achinyamata angachite chiyani kuti makolo awo aziwakhulupirira ndi kuwalemekeza?
[Mawu a Chithunzi patsamba 3]
© Jacob Silberberg/Panos Pictures