Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

July 2008

Kodi mungatani kuti banja lanu liziyenda bwino?

Mabanja ambiri nthawi zina amayenda bwino, koma nthawi zina amakumana ndi zovuta. Ndiye kodi mungatani kuti banja lanu likhale losangalala ndi lolimba? Baibulo lili ndi mfundo zothandiza kwambiri pankhaniyi.

3 Mabanja Ali pa Vuto

4 N’chiyani Chimayambitsa Mavutowo?

6 Zimene Mungachite Kuti Banja Lanu Liziyenda Bwino

12 Kodi Dzikoli Lidzakhalabe ndi Zinthu Zokwanira Anthu Onse?

18 Kadziweni Kanyama Aka

19 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndingatani Kuti Kulambira Mulungu Kuzindisangalatsa?

22 Chakudya cha ku Thailand

24 Tizigoba Tokongola ta ku Niihau

26 M’kamwa

Munapangidwadi Mwaluso

27 Vuto Lokhala Alubino

30 Zochitika Padzikoli

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 “Bukuli Ndi Labwino Kwambiri!”

N’chifukwa Chiyani Muyenera Kupewa Zamizimu? 10

Anthu ambiri amachita zinthu zokhulupirira mizimu chifukwa cha chidwi basi. Koma kodi kuopsa kwake n’kotani? Kodi Mulungu amaiona bwanji nkhani yokhulupirira mizimu?

Ngalande za ku Britain Zikuchititsabe Chidwi 13

Ngalande zimenezi zinakumbidwa m’ma 1800, ndipo kenako anasiya kuzigwiritsa ntchito. Panopa azikonzanso moti zikukopa alendo ambiri okaona malo.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Courtesy of British Waterways