Kodi Mungayankhe Bwanji?
Kodi Mungayankhe Bwanji?
Kodi Zinachitikira Kuti?
1. Kodi Yesu ananyamukira kuti popita kumwamba?
ZOKUTHANDIZANI: Werengani Machitidwe 1:6-12.
Lembani mzere wozungulira yankho lanu pamapupo.
Phiri la Karimeli
Phiri la Gerizimu
Phiri la Maolivi
Hebroni
▪ Yesu atatsala pang’ono kupita kumwamba, ophunzira ake anamufunsa chiyani?
․․․․․
▪ Kodi Yesu anati ophunzira ake adzatani?
․․․․․
KAMBIRANANI:
Kodi mawu a angelo a pa Machitidwe 1:11 akwaniritsidwa bwanji? Kodi mungatani kuti muzichita nawo ntchito imene Yesu anauza otsatira ake, monga momwe zalembedwera pa Machitidwe 1:8?
Kuchokera M’magazini Ino
Yankhani mafunsowa, ndipo lembani vesi kapena mavesi a m’Baibulo omwe akusowapo.
TSAMBA 4 Kodi Baibulo limanena chiyani za Eliya? Yakobe 5:․․․
TSAMBA 7 Kodi munthu amakhala ndi moyo ndi chiyani? Mateyo 4:․․․
TSAMBA 19 Kodi ndani amapambana mbale kuumirira? Miyambo 18:․․․
TSAMBA 20 Kodi pali nthawi yochita chiyani? Mlaliki 3:․․․
Zithunzi Zoti Ana Apeze
Kodi mungapeze zithunzi izi m’magazini ino? Fotokozani zimene zikuchitika pa chithunzi chilichonse.
Ndani Ali M’gulu la Makolo a Yesu?
Onani zokuthandizani kupeza yankho. Onaninso malembawo. Kenaka lembani mayina olondola pa mizereyi.
2. ․․․․․
ZOKUTHANDIZANI: Panthawi ya ulamuliro wanga, Hilikiya “anapeza buku la chilamulo la Yehova mwa dzanja la Mose.”
Werengani 2 Mbiri 34:1, 14.
3. ․․․․․
ZOKUTHANDIZANI: Ndinali chiwanga kapena kuti kazembe woyamba wa Ayuda amene anabwerera ku Isiraeli kuchoka ku Babulo.
Werengani Hagai 1:14.
4. ․․․․․
ZOKUTHANDIZANI: Ntchito yanga inali yopala matabwa.
Werengani Mateyo 1:16; 13:55.
▪ Mayankho ali pa tsamba 14
MAYANKHO A MAFUNSO A PA TSAMBA 31
1. Phiri la Maolivi.
▪ Anamufunsa Yesu nthawi imene adzabwezeretse Ufumu.
▪ Yesu anati ophunzira ake adzalalikira za iye mpaka kumalekezero a dziko lapansi.
2. Yosiya.—Mateyo 1:10.
3. Zerubabele.—Mateyo 1:12.
4. Yosefe.—Mateyo 1:16.
[Mawu a Chithunzi patsamba 31]
Center circle: Oxford Scientific/photolibrary