Mlozera Nkhani Wa Magazini a Galamukani! a 2009
Mlozera Nkhani Wa Magazini a Galamukani! a 2009
CHIPEMBEDZO
Achinyamata a Katolika Anauzidwa Kuti Azilalikira, 6/09
Dzina la Mulungu ku Denmark, 11/09
Nyenyezi Imene Inatsogolera “Anzeru a Kum’mawa,” 12/09
MAUNANSI A ANTHU
Achinyamata Kodi Mungathane Bwanji ndi Mavuto Anu? 9/09
Ana Ambiri Akumapanikizika, 5/09
Anthufe Ndi Amodzi, 11/09
Kalankhulidwe Kogometsa Koimba Likhweru, 2/09
Kodi Kutha kwa Banja Kumakhudza Bwanji Ana? 10/09
Kodi Tsankho Limayamba Bwanji? 8/09
Kuthandiza Ana Amene Ali Ndi Vuto Lophunzira, 1/09
Mfundo Zothandiza Kuti Banja Lanu Liziyenda Bwino, 10/09
N’zotheka Kulera Nokha Ana, 10/09
Thandizani Ana Anu Kuti Akule Bwino, 6/09
Ubwino Wosonyezana Chikondi, 12/09
MAYIKO NDI ANTHU
Akapolo Oiwalidwa a ku South Pacific, 1/09
Albarracín Ndi Tawuni Yokongola Kwambiri (Spain), 7/09
Anthu Otcheza Mchere ku Sahara, 1/09
“Dera Loiwalika” la ku Bolivia, 11/09
Dzina la Mulungu ku Denmark, 11/09
Galimoto Yopalasa? (Bangladesh), 7/09
Mankhwala Odzikongoletsera Ochokera ku Mitengo (Madagascar), 7/09
Mzinda wa Bucharest(Romania), 4/09
Mzinda wa Plovdiv (Bulgaria), 6/09
Nyama ndi Zomera Zikutha (Spain), 3/09
MBIRI YA MOYO WA ANTHU
Chimene Chinandichititsa Kusiya Kukonda Nkhondo (T. Stubenvoll), 12/09
Ndakhala Wokhulupirika kwa Zaka Zoposa 70 (J. Elias), 9/09
Ndinamasulira Mabuku Mobisa kwa Zaka 30 (O. Mockutė), 6/09
Ndinasiya Usilikali N’kuyamba Kutumikira Yehova (A. Hogg), 11/09
Ndinathawa Nkhondo (S. Tan), 5/09
Sindinabwerere M’mbuyo Ngakhale Kuti Ndili ndi Matenda Olepheretsa Kuwerenga (M. Henborg), 2/09
Tinadalitsidwa Chifukwa Chokonda Kwambiri Mulungu (P. Worou), 3/09
Tinapeza Zimene Tinkafuna (B. Tallman), 1/09
MBONI ZA YEHOVA
Analimba Mtima Kufotokoza Zimene Amakhulupirira, 12/09
‘Chitseko Chimene Yehova Yekha Ndi Amene Angatsegule’ (manda), 8/09
Kabuku Kanga Kapinki (buku la Mphunzitsi Wamkuruyo), 3/09
Kugwiritsitsa Dzanja Lamanja la Mulungu (matenda a pakhungu), 9/09
‘Limayankha Mafunso Athu’ (Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri), 7/09
Mphunzitsi Anasintha Maganizo Ake (Georgia), 3/09
Msonkhano Wachigawo wa “Khalani Maso,” 5/09, 6/09
Wodwala Ali Ndi Ufulu Wosankha, 6/09
Zimene Mukufuna Zili M’Baibulo, 11/09
SAYANSI
Chigoba cha Chikumbu, 5/09
Dzikoli Linapangidwa Kuti Likhale ndi Zamoyo, 2/09
Kachipangizo Kochititsa Chidwi, 3/09
Kodi Mumatha Kusunga Zinthu Zanu Mwachinsinsi? 8/09
Kufika ku Mars, 2/09
Kumwamba Kuli Zinthu Zambiri Zodabwitsa, 8/09
Mapiko a Zamoyo Zouluka, 2/09
Masamba a Kakombo, 4/09
Mlomo wa Mbalame Yotchedwa Toucan, 1/09
Mlomo Wochititsa Chidwi wa Nyama ya M’madzi, 3/09
N’chifukwa Chiyani Mulungu Analenga Zonsezi? 12/09
Nthenga za Kadzidzi, 12/09
N’zotheka Ndithu Kuchepetsa Vuto la Kuiwala, 2/09
Umboni Wosonyeza Kuti Nkhani za M’Baibulo N’zoona, 5/09
Woyamba Kujambula Mapu a Dziko Lonse (Mercator), 4/09
Zigoba za Nkhono Zam’madzi, 8/09
Zipangizo Zamakono, 11/09
UMOYO NDI MANKHWALA
Anthu Ovutika Maganizo, 7/09
Kodi Kukachitika Ngozi Mumadziwitsa Ndani? 4/09
Kodi Mungatani Kuti Mwana Wanu Asanenepe Kwambiri? 3/09
Kuchotsa Mimba, 6/09
Kugwiritsa Ntchito Mankhwala Moyenera, 5/09
Kukhalitsa Padzuwa, 6/09
Matenda a Chithokomiro, 5/09
Mayi Wathanzi Amaberekanso Mwana Wathanzi, 11/09
Samalani ndi Poizoni, 12/09
ZACHUMA NDI NTCHITO
Kodi Ndinu Kapolo wa Ndalama? 3/09
Njinga Yonolera Mipeni, 2/09
ZIMENE ACHINYAMATA AMADZIFUNSA
Kodi Ndingatani Kuti Ndidziwane Bwino Ndi Makolo Anga? 10/09
Kodi Ndingatani Kuti Ndimuiwale? 2/09
Kodi Ndingatani Kuti Ndizilankhula Momasuka ndi Makolo Anga? 12/09
Kodi Ndingatani Kuti Ndizipewa Kupsa Mtima? 9/09
Kodi Ndingatani Ngati Kholo Langa Lamwalira? 8/09
Kodi Ndipeze Anzanga Ena Abwino? 3/09
Kodi Ndithetse Chibwenzi? 1/09
Kodi Ndizivala Bwanji? 11/09
N’chifukwa Chiyani Atsikana Amangondikana? 5/09
N’chifukwa Chiyani Ndimaopa Kuuza Ena za Chikhulupiriro Changa? 7/09
Ndingatani Kuti Kuwerenga Baibulo Kuzindisangalatsa? 4/09
Ndingatani Kuti Ndizigwiritsa Ntchito Nthawi Moyenera? 6/09
ZIMENE BAIBULO LIMANENA
Kodi Abusa Ndi Apamwamba Kuposa Anthu Ena Mumpingo?
Kodi Anthu Oipa Adzakapsa Kumoto? 9/09
Kodi Kukhulupirika M’banja N’kutani? 4/09
Kodi Kutentha Mtembo N’kulakwa? 3/09
Kodi Mulungu Amafuna Kuti Mukhale Wolemera? 5/09
Kodi Mungathetse Bwanji Njala Yanu Yauzimu? 12/09
Kodi Muyenera Kuopa Anthu Akufa? 6/09
Kodi N’kulakwa Mwamuna ndi Mkazi Kukhalira Limodzi Asanakwatirane? 10/09
Kodi N’zotheka Kukonda Adani Athu? 11/09
Kodi Tikamavutika Ndiye Kuti Mulungu Akutilanga? 1/09
Kodi Tsogolo Lanu Linalembedweratu? 2/09
Kusintha Chipembedzo Chanu N’kulakwa? 7/09
ZINYAMA NDI ZOMERA
Chigoba cha Chikumbu, 5/09
Kanyama Kaulesi, 7/09
Kuphunzitsa Njovu, 4/09
Makolo Ogwirizana, 8/09
Mapiko a Zamoyo Zouluka, 2/09
Masamba a Kakombo, 4/09
Mbalame Zimawomba Makoma Mwangozi, 2/09
Mlomo Wochititsa Chidwi wa Nyama ya M’madzi, 3/09
Njovu Zikuluzikulu Zinkapezeka Paliponse ku Ulaya, 5/09
Nsomba Yochititsa Chidwi, 7/09
Nthenga za Kadzidzi, 12/09
Nyama ndi Zomera Zikutha (Spain), 3/09
Nyama Zikuluzikulu za M’nyanja, 12/09
Mlomo wa Mbalame Yotchedwa Toucan, 1/09
Ulimi Wamakono, 9/09
Zigoba za Nkhono Zam’madzi, 8/09
Zipatso Zofunika Kwambiri, 9/09
Ziwombankhanga Zikuluzikulu, 5/09
ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE
Achinyamata Kodi Mungathane Bwanji ndi Mavuto Anu? 9/09
Kodi Madzi Akutha Padzikoli? 1/09
N’chifukwa Chiyani Anthu Amasankhana? 8/09
N’chiyani Chinayambitsa Nkhondo ya Padziko Lonse? 8/09
Ulimi Wamakono, 9/09
ZOSIYANASIYANA
Herode Anali Katswiri pa Zomangamanga, 9/09
Kamvuluvulu Wapanyanja, 9/09
Luso Lopanga Khofi, 8/09
Mungatani Kuti Muziyendetsa Bwino Galimoto? 7/09
Mungatani Ngati Mumapanikizika ndi Sukulu Ndiponso Zinthu Zina? 4/09
Pizza, 1/09