Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mawu Oyamba

Mawu Oyamba

KODI MALANGIZO OTHANDIZA KUTI TIZIKHALA OSANGALALA TINGAWAPEZE KUTI?

Baibulo limanena kuti: “Odala ndi anthu osalakwitsa kanthu m’njira zawo.”​—Salimo 119:1.

Nkhani zokwana 7 zomwe zili m’magaziniyi zikufotokoza zimene tingachite kuti tizikhala osangalala.