Mawu Oyamba
KODI MALANGIZO OTHANDIZA KUTI TIZIKHALA OSANGALALA TINGAWAPEZE KUTI?
Baibulo limanena kuti: “Odala ndi anthu osalakwitsa kanthu m’njira zawo.”—Salimo 119:1.
Nkhani zokwana 7 zomwe zili m’magaziniyi zikufotokoza zimene tingachite kuti tizikhala osangalala.