Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mawu Oyamba

Mawu Oyamba

Anthu ambiri padzikoli amadana ndipo amachita zinthu zankhanza zambirimbiri. Mwachitsanzo, amasala ena, kuwachitira nkhanza, kuwalankhula mawu achipongwe kapenanso kuwavulaza. Kodi chidani chidzatha? Nkhani zomwe zili m’magaziniyi zitithandiza kuona mmene Baibulo lingatithandizire kuthetsa chidani. Tionanso zomwe Mulungu analonjeza zoti adzathetseratu chidani.