Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! a 2019

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! a 2019

Wosonyeza deti la magazini imene muli nkhaniyo

NSANJA YA OLONDA YOPHUNZIRA

BAIBULO

  • Akwanitsa Kuwerenga Mpukutu Wakale, June

MAFUNSO OCHOKERA KWA OWERENGA

  • Kodi zoti mzimu suufa zinayambira mu Edeni? (Ge 3:4), Dec.

  • N’chifukwa chiyani mtsikana wogwiriridwa “kuthengo” sankaimbidwa mlandu ngakhale kuti panalibe mboni ziwiri? (De 22:25-27), Dec.

MBIRI YA MOYO WANGA

  • Makolo Anga Anandithandiza Kuti Ndizitumikira Yehova (W. Mills), Feb.

  • Tinapeza ‘Ngale Yamtengo Wapatali’ (W. ndi P. Payne), Apr.

  • Yehova Wandidalitsa Kuposa Mmene Ndinkaganizira (M. Tonak), July

MBONI ZA YEHOVA

  • 1919​—Zaka 100 Zapitazo, Oct.

  • M’bale Watsopano M’bungwe Lolamulira (K. Cook, Jr.), Jan.

MOYO NDI MAKHALIDWE ACHIKHRISTU

  • Chikhulupiriro Chimatipatsa Mphamvu, Aug.

  • Chitsanzo Chabwino pa Nkhani Yokhalabe Wosangalala (Yohane M’batizi), Aug.

  • “Muziyamika pa Chilichonse,” Dec.

  • Ubwino​—Kodi Tingatani Kuti Tikhale ndi Khalidweli? Mar.

NKHANI ZOPHUNZIRA

  • Aisiraeli Ankafunika Kusonyeza Chikondi ndi Chilungamo, Feb.

  • “Anthu Okumvera” Adzapulumuka, Aug.

  • “Bwerani kwa Ine . . . Ndipo Ndidzakutsitsimutsani,” Sept.

  • Chikondi Chanu Chipitirire Kukula, Aug.

  • Chikundiletsa Kubatizidwa N’chiyani? Mar.

  • Kodi Mukukwaniritsa Mbali Zonse za Utumiki Wanu? Apr.

  • Kodi Mukusamalira ‘Chishango Chanu Chachikulu Chachikhulupiriro’? Nov.

  • Kodi Mumamudziwa Bwino Yehova? Dec.

  • Kodi Mzimu Woyera Umatithandiza Bwanji? Nov.

  • Kodi Tingateteze Bwanji Mtima Wathu? Jan.

  • Kodi Tingathandize Bwanji Anthu Amene Sakonda Zachipembedzo? July

  • Kodi Yehova Adzakuthandizani Kuchita Chiyani? Oct.

  • Lolani Kuti Yehova Akuthandizeni Polimbana ndi Mizimu Yoipa, Apr.

  • Makhalidwe Amene Amatichititsa Kupezeka Pamisonkhano, Jan.

  • Makolo Ayenera Kuphunzitsa Ana Awo Kukonda Yehova, Dec.

  • “Malizitsani” Zimene Munayamba Kuchita, Nov.

  • Muziyesetsa Kuti Kuphunzira Kuzikuthandizani, May

  • Mwambo wa Chikumbutso Umasonyeza Makhalidwe a Mfumu Yakumwamba, Jan.

  • “Ndinaona Khamu Lalikulu la Anthu,” Sept.

  • Pali Nthawi Yogwira Ntchito ndi Nthawi Yopuma, Dec.

  • Pezani Anzanu Apamtima Mapeto Asanafike, Nov.

  • ‘Pitani Mukaphunzitse Anthu Kuti Akhale Ophunzira Anga,’ July

  • Pitirizani Kukhala ndi Mtima Wosagawanika, Feb.

  • ‘Samalani Kuti Wina Angakugwireni,’ June

  • “Sitikubwerera M’mbuyo,” Aug.

  • Tidzakhalebe Okhulupirika pa “Chisautso Chachikulu,” Oct.

  • Tisapusitsidwe ndi “Nzeru za M’dzikoli,” May

  • Tizichita Zinthu Moganizira Ena, Mar.

  • Tizichotsa Maganizo Alionse Otsutsana ndi Kudziwa Mulungu, June

  • Tizidalira Yehova Tikakhala ndi Nkhawa, June

  • Tizigonjera Yehova ndi Mtima Wonse, Sept.

  • Tizikhala Odzipereka kwa Yehova Yekha, Oct.

  • Tizikonzekera Kuti Tidzathe Kupirira Pozunzidwa, July

  • Tizilambirabe Yehova Ngakhale Boma Litatiletsa, July

  • Tizilimbikitsa Anthu Amene Achitiridwa Zoipa, May

  • Tizimvetsera Mawu a Yehova, Mar.

  • Tizisonyeza Anthu Chifundo Tikakhala mu Utumiki, Mar.

  • Tizisonyeza Chikondi ndi Chilungamo M’dziko Loipali, May

  • Tizisonyeza Chikondi ndi Chilungamo Mumpingo, May

  • Tizisonyeza Kuti Ndife Oyamikira, Feb.

  • Tizitamanda Yehova Mumpingo, Jan.

  • Tizithandiza Anthu Amene Ali ndi Nkhawa, June

  • Tizitsanzira Yesu Kuti Tizikhala ndi Mtendere Wamumtima, Apr.

  • Tizitsatira Mfundo za Choonadi Pakachitika Maliro, Apr.

  • Tizitumikira Yehova Mwakhama Kumapeto kwa ‘Masiku Otsirizawa,’ Oct.

  • “Usayang’ane Uku ndi Uku Mwamantha, Pakuti Ine Ndine Mulungu Wako,” Jan.

  • Uthenga Wokhudza Aramagedo Ndi Wosangalatsa, Sept.

  • Yehova Amaona Kuti Atumiki Ake Odzichepetsa Ndi Amtengo Wapatali, Sept.

  • Yehova Anakonza Zoti Tikhale ndi Ufulu, Dec.

  • Yesetsani Kukhala Ofatsa Kuti Muzisangalatsa Yehova, Feb.

  • Zimene Tingachite Kuti Tizisangalalabe Utumiki Wathu Ukasintha, Aug.

  • Zimene Tingaphunzire M’buku la Levitiko, Nov.

NKHANI ZOSIYANASIYANA

  • Kodi Ankayenda Bwanji Panyanja? Apr.

  • Kodi Masunagoge Anayamba Bwanji? Feb.

  • Msampha Wina wa Satana (zolaula), June

  • Mtumiki Woyang’anira Nyumba, Nov.

YEHOVA

  • Kodi Amachenjeza Mokwanira? Oct.

  • Mawu Akuti “Ame,” Mar.

YESU KHRISTU

  • Kodi N’zoona Kuti Anandifera Ineyo? July

NSANJA YA OLONDA YOGAWIRA

  • Kodi Mukuona Kuti Palibenso Chifukwa Chokhalira ndi Moyo? Na. 2

  • Kodi Mulungu Ankafuna Kuti Tizikhala ndi Moyo Waufupi Chonchi? Na. 3

  • Kodi Mulungu Ndi Ndani? Na. 1

GALAMUKANI!

  • Baibulo Lingakuthandizeni Kukhala ndi Moyo Wabwino Kwambiri, Na. 3

  • Kodi Tingadzakhaledi Otetezeka Padzikoli? Na. 1

  • Makhalidwe 6 Amene Muyenera Kuphunzitsa Ana Anu, Na. 2