NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA) September 2018
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira pa October 29 mpaka December 2, 2018
“Ngati Zimenezi Mukuzidziwa, Ndinu Odala Mukamazichita”
Kodi tingatani kuti tikhalebe odzichepetsa, nanga n’chifukwa chiyani tiyenera kuchita zimenezi?
Akhristu Achikulire, Yehova Amayamikira Kukhulupirika Kwanu
Kodi akulu achikulire a masiku ano asonyeza bwanji kudzichepetsa?
Pitirizani Kusonyeza Chikondi Chifukwa Chimalimbikitsa
Onani zimene tingachite kuti tizilimbikitsana m’masiku ovuta ano.
Anthu Amene Amatumikira “Mulungu Wachimwemwe” Amakhala Osangalala
Kodi tingatani kuti tizikhalabe achimwemwe ngakhale kuti timakumana ndi mavuto?
Nthawi Ili Bwanji?
Kodi anthu otchulidwa m’Baibulo ankatchula bwanji nthawi?
Yehova Ndi Wamphamvuyonse Koma Amaganizira Ena
Kodi Yehova amapereka bwanji chitsanzo chabwino pa nkhani yochita zinthu moganizira ena?
Tizikhala Okoma Mtima Komanso Oganizira Ena Ngati Yehova
Phunzirani njira zimene tingasonyezere kuti timaganizira ena m’banja, mumpingo komanso mu utumiki.