Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Kalozera wa Nkhani za M’magazini a Nsanja ya Olonda a 2005

Kalozera wa Nkhani za M’magazini a Nsanja ya Olonda a 2005

Kalozera wa Nkhani za M’magazini a Nsanja ya Olonda a 2005

Wosonyeza deti la magazini yopezekamo nkhaniyo

BAIBULO

Baibulo la Berleburg, 2/15

Baibulo Lachifumu, 8/15

Baibulo Lakale la Chijeremani Lili ndi Dzina la Mulungu, 9/1

Buku Lothandiza Pantchito Yomasulira Mabuku, 4/15

Chitaliyana​—Mavuto Amene Lakumana Nawo, 12/15

Kodi Mbiri ya M’Baibulo N’jolondoladi? 4/15

Laibulale Yakale Kwambiri ya ku Russia Ithandiza ‘Kumvetsetsa’, 7/15

Lingakuthandizeni Kukhala Wosangalala, 8/1

Mfundo Zazikulu za M’buku la Oweruza, 1/15

Mfundo Zazikulu za M’buku la Rute, 3/1

Mfundo Zazikulu za M’buku la Samueli Woyamba, 3/15

Mfundo Zazikulu za M’buku la Samueli Wachiwiri, 5/15

Mfundo Zazikulu za M’buku la Mafumu Woyamba, 7/1

Mfundo Zazikulu za M’buku la Mafumu Wachiwiri, 8/1

Mfundo Zazikulu za M’buku Loyamba la Mbiri, 10/1

Mfundo Zazikulu za M’buku Lachiwiri la Mbiri, 12/1

Muyezo wa “Pimu” Ukutsimikizira Kuti Baibulo ndi Lolondola Mogwirizana ndi Mbiri Yakale, 3/15

Nyanja ya Galileya (ancient boat), 8/15

Sayansi ndi, Zimatsutsanadi? 4/1

“Vuto Lija Latha Tsopano” (New World Translation of Christian Greek Scriptures mu Chilingala), 7/1

Ziphunzitso Zoona, 7/15

KALENDALA

Achinyamata Amene Amatamanda Yehova Amakhala ndi Moyo Wabwino, 3/15

Anthu Ochuluka Ayamba Kupembedza Yehova, 9/15

Anthu Odzimana, 11/15

Mabanja Odziwa Mulungu Amalimba, 5/15

Osakwatira Koma Osangalala, 7/15

Ukalamba Umene Uli “Korona wa Ulemu,” 1/15

MAFUNSO OCHOKERA KWA OWERENGA

Amene Iye yekha ali nawo moyo wosatha,” ndiponso “amene munthu sanamuona, akunena za Yesu? (1Ti 6:15, 16), 9/1

Davide ankachitira nkhanza anthu omwe anawagwira kunkhondo? 2/15

Davide ndi anyamata ake adya mkate wopatulika, 3/15

“Kapena” (Zef 2:3), 8/1

Kutsutsana ndi kudya kwa mtembo wake? (Lev 11:40; De 14:21), 7/1

Masewera achiwawa a pakompyuta, 9/15

Mkazi wachikristu “adzapulumutsidwa mwa kubala mwana” (1Ti 2:15), 5/1

Mngelo wa Petro (Mac 12:15), 6/1

Mphatso kwa munthu wogwira ntchito m’boma? 4/1

N’chifukwa chiyani Davide ndi Bateseba sanaphedwe? 5/15

Ntchito yofunika kuti azinyamula mfuti, 11/1

Paulo: “Ine ndine Mfarisi” (Mac 23:6), 4/15

Samsoni agwira mitembo ya anthu amene anapha koma n’kupitirizabe kukhala Mnaziri? 1/15

Samsoni anang’amba mkango “monga akadang’amba mwana wa mbuzi,” 1/15

Shekina m’Chipinda Chopatulikitsa, 8/15

Solomo adzauka kwa akufa? 7/15

Stefano apemphera kwa Yesu? 1/1

MBIRI YA MOYO WANGA

Chitsanzo cha Makolo Anga Chinandilimbitsa (J. Rekelj), 10/1

Kupirira Monga Msilikali wa Kristu (Y. Kaptola), 9/1

Kusangalala Nawo “Moyo Uno” (T. Buckingham), 6/1

Mwana Wamasiye Wosowa Wom’samala Apeza Atate Womukonda (D. Sidiropoulos), 4/1

Ndinalandira ‘Zokhumba Mtima Wanga’ (D. Morgou), 11/1

Ndine Wamphamvu Ngakhale Ndili Wofooka (L. Engleitner), 5/1

Ndine Wosangalala Kuti Ndagwira Nawo Ntchito ya Padziko Lonse Yophunzitsa Baibulo (A. Matheakis), 7/1

Sindidzasiya Kutumikira Mlengi Wanga (C. Benanti), 12/1

Tinachita Zazikulu (E. Ludolph), 5/1

Tinalalikira M’madera Akutali Chifukwa Chosamukasamuka (R. Malicsi), 3/1

Tinaphunzira Kukhulupirira Yehova ndi Mtima Wonse (N. Holtorf), 1/1

Yehova Amadalitsa Kwambiri (R. Stawski), 8/1

MBONI ZA YEHOVA

“Akanamasulidwa Mosavuta,” 8/15

Amalalikira Uthenga Wabwino kwa Ogontha (Spain), 11/1

Amenoni Afunafuna Choonadi (Bolivia), 9/1

“Anazunzidwa Chifukwa cha Chikhulupiriro Chake” (N. Riet), 6/15

Anthu Oona Mtima, 6/1

‘Chikondano cha Inu Nonse Chikukula’ (Japan), 11/15

Chiyembekezo Chimalimbikitsa, 3/1

“Dziko la Chiwombankhanga” (Albania), 10/15

Khalidwe Labwino Limabala Zipatso Zabwino (Japan), 11/1

“Kukhulupirika M’nthawi ya Mayesero” (vidiyo), 3/1

“Kulalikira Am’nsinga Mamasulidwe” (ntchio ya ku ndende), 12/15

Kutamanda Yehova ku Sukulu, 6/15

Kuthandiza Anthu a ku China Omwe Akukhala ku Mexico, 12/15

“Limodzi mwa Masiku Amene Ndinasangalala Kwambiri Pamoyo Wanga” (Australia), 11/1

Macedonia, 4/15

M’madera a Kumidzi ku Australia, 4/1

Mphamvu ya Mawu a Mulungu, 2/15

Msonkhano Umene Unachitika mu Msasa wa Anthu Othawa Kwawo (Kenya), 4/15

Mwambo Womaliza Maphunziro a Gileadi, 7/1

Ntchito Yolalikira Ikupita Patsogolo ku Dziko Limene Kale Chikristu Chinali Kuyenda Bwino (Italy), 6/15

Saba, 2/15

“Sanasiye Chikhulupiriro Chawo,” 7/15

Umboni wa Chikondi, Chikhulupiriro, ndi Kumvera (Nyumba Yosindikizira ku Watchtower Farms), 12/1

“Uthenga Wabwino wa Anthu a Mitundu Yonse” (kabuku), 12/1

Zopereka, 11/1

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Chikhulupiriro Chanu Chimakulimbikitsani Kuchitapo Kanthu? 4/15

Kodi Chikumbumtima Chanu Ndi Chophunzitsidwa Bwino? 10/1

Kodi Choonadi Chikubala Zipatso Mwa Anthu Amene Mumawaphunzitsa? 2/1

Kodi Kukhumudwa Koyenera N’kotani? 8/1

Kodi Mukumanga pa Maziko Otani? 5/15

Kodi Muli “Nacho Chuma cha kwa Mulungu”? 10/1

Kodi Mumacheza Nawo Okondedwa Anu? 6/1

Kodi Mumadziyerekezera ndi Ena? 2/15

Kodi Ndi Bwino Kuganizira Mmene Ena Amationera? 9/15

Kukhala Wokhulupirika, 9/1

Kulimba Mtima Povutitsidwa, 5/1

Kumvetsera Mwachikondi, 11/15

Kuopa Yehova Ndiko Nzeru (Miy 14), 9/15

Kupindula ndi Tsiku Lililonse, 5/1

“Mawu” a Yehova Azikutchinjirizani, 9/1

M’banja Mukabuka Mikangano, 6/1

Miyambo Imene Mulungu Sakondwera Nayo, 1/1

Mmene Mungatetezere Ana Anu ndi Nzeru za Mulungu, 1/1

“Mucherezane Wina ndi Mnzake,” 1/15

Musaleme Pakuchita Zabwino, 6/1

N’chifukwa Chiyani Ambiri Amalephera Kulingalira Bwino? 5/15

Nthawi Yachakudya, 1/1

Pewani Maganizo Olakwika, 9/15

Tingapirire Mayesero Alionse, 6/15

Ubwino Wokhazikitsa Mtendere, 3/1

“Wochenjera Asamalira Mayendedwe Ake” (Miy 14), 7/15

Yehova Sadzakusiyani Konse, 10/15

Zimene Mungachite Kuti Yehova Akhale Mulungu Wanu, 4/1

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA

Akristu Amawalitsa Ulemerero wa Yehova, 8/15

Ana Athu Ndi Cholowa Chamtengo Wapatali, 4/1

Ananu, Tamandani Yehova! 6/15

Anthu “a Manenedwe Onse” Akumva Uthenga Wabwino, 12/1

Chiphunzitso cha Kuuka kwa Akufa Chimakukhudzani, 5/1

“Dikirani” Chifukwa Nthawi ya Chiweruzo Yafika, 10/1

‘Dzitsimikizireni Nokha,’ 7/15

Ino ndi Nthawi Yofunika Kuchitapo Kanthu Mwachangu, 12/15

Khalani Odzichepetsadi, 10/15

Khulupirirani Mawu a Yehova, 4/15

Kodi Chiyembekezo cha Kuuka kwa Akufa Mumachiona Motani? 5/1

Kodi Inuyo Mumamvera Ndani​—Mulungu Kapena Anthu? 12/15

Kodi Mudzawalitsa Ulemerero wa Mulungu? 8/15

Kodi Muyenda ndi Mulungu? 11/1

Kodi Ndinu Wokhulupirika M’zinthu Zonse? 7/15

Kufalitsa “Uthenga Wabwino wa Zinthu Zabwino,” 7/1

Kufunafuna ‘Ngale ya Mtengo Wapatali’ Lerolino, 2/1

Kukhala Atumiki Opita Patsogolo ndi Otha Kusintha, 12/1

‘Kupeza Ngale Imodzi ya Mtengo Wapatali,’ 2/1

Kuteteza Dzina Lathu Monga Akristu, 2/15

Lamulo la Chikondi Lolembedwa M’mitima, 8/15

Lolani Kuti Mawu a Mulungu Aunike Njira Yanu, 4/15

Makolo​—Kodi Ana Anu Mukuwafunira Tsogolo Lotani? 10/1

Makolo, Pezerani a M’banja Lanu Zosowa Zawo, 6/15

Makolo, Tetezani Cholowa Chanu Chamtengo Wapatali, 4/1

Malangizo Anzeru kwa Okwatirana, 3/1

Masomphenya a Ufumu wa Mulungu Asanduka Zenizeni, 1/15

Maulosi a Baibulo Agona pa Kristu, 1/15

“Munagulidwa ndi Mtengo Wake Wapatali,” 3/15

Ndani Adzaukitsidwe? 5/1

“Njira za Yehova Zili Zoongoka,” 11/15

Nyadirani Kuti Ndinu Mkristu! 2/15

Phunzirani Njira za Yehova, 5/15

Pitirizani Kuyenda Monga Yesu Kristu Anayendera, 9/15

Samalani Kuti Musakhale ndi Mtima Wodzikuza, 10/15

Taphunzitsidwa Kuchitira Umboni Mokwanira, 1/1

Tidzapulumuka mwa Chisomo Osati mwa Ntchito Zokha, 6/1

Tidzayenda M’dzina la Yehova Mulungu Wathu, 9/1

Tisakhalenso ndi Moyo Mwa Ife Tokha, 3/15

Tsatirani Chitsanzo Chimene Yesu Anatipatsa, 1/1

‘Ugwireni Mtima Pokumana ndi Zoipa,’ 5/15

Ukwati Ungayende Bwino Masiku Ano, 3/1

Ulosi wa Hoseya Umatithandiza Kuyenda ndi Mulungu, 11/15

Uthenga Wabwino wa Anthu a Mitundu Yonse, 7/1

Yehova Amasunga Anthu Amene Amamudalira, 6/1

Yehova Amawerenga ‘Tsitsi Lonse la M’mutu Mwanu,’ 8/1

Yehova Ndi Mbusa Wathu, 11/1

Yehova Ndi “Wobwezera Mphoto Iwo Akum’funa Iye,” 8/1

Yendani mwa Chikhulupiriro Osati mwa Zooneka ndi Maso, 9/15

Yendani ndi Mulungu, Kuti Mukolole Zabwino, 11/15

Yendani ndi Mulungu M’nthawi ya Chipwirikiti Ino, 9/1

NKHANI ZOSIYANASIYANA

‘Akakukakamizani’ Kuchita Zinthu’ (Mt 5:41), 2/15

Angasinthedi Dzikoli? 11/1

Armagedo, 12/1

Chifukwa Chake Anthu Ambiri Amakayikira Zoti Zipembedzo Zingagwirizanitse Anthu Onse? 1/1

Chilengedwe Chodabwitsachi Chimatamanda Yehova, 11/15

Chiyembekezo cha Kuuka kwa Akufa, 5/1

Chizindikiro cha Kukhalapo kwa Yesu, 10/1

Dipo Limasonyeza Bwino Chilungamo cha Mulungu, 11/1

Filo wa ku Alexandria, 6/15

Imfa, 8/15

‘Iwo Akutsikira Kunyanja M’zombo,’ 10/15

Kodi Moyo Wanu Ndi Wamtengo Wapatali Motani? 2/1

Kodi Nkhani Yaikulu Panyengo ya Khirisimasi Imakhala Chiyani? 12/15

Kodi Ntchito Ndi Dalitso Kapena Temberero? 6/15

Kodi Tsogolo Lanu Linakonzedweratu? 1/15

Kufalikira kwa Chikristu Pakati pa Ayuda M’nthawi ya Atumwi, 10/15

Kufunafuna Mtendere wa Mumtima, 7/1

Kulalikira kwa Saulo Kunamudanitsa ndi Anthu, 1/15

Kuphunzira Panopa Mpaka Muyaya, 4/15

“Lupanga la Yehova ndi la Gideoni,” 7/15

Maphunziro Abwino Koposa, 10/15

Mari​—Mzinda Wakale Wotchuka wa M’chipululu, 5/15

Mdyerekezi Alikodi? 11/15

Mgwirizano wa Padziko Lonse, 6/1

‘Ngati Mwala Wofiira Wamtengo Wapatali’ (Chi 4:3), 3/15

Nyengo ya Tchuthi, 12/15

Pontiyo Pilato, 9/15

Samsoni Anapambana Chifukwa cha Mphamvu za Yehova, 3/15

Umphawi, 5/15

Ziphunzitso Zoona, 7/15

Zozizwitsa, 2/15

YEHOVA

Yehova Amachita Chilungamo Nthawi Zonse, 2/1

YESU KRISTU

Kodi Yesu Kristu Ndani? 9/15

Kodi Ziphunzitso za Yesu Kristu Zimakukhudzani Motani? 3/15