Zamkatimu
Zamkatimu
May 15, 2008
Magazini Yophunzira
NKHANI ZOPHUNZIRA MLUNGU WA:
June 30, 2008–July 6, 2008
Kodi Tizikhala Bwanji ndi Anzathu?
TSAMBA 3
NYIMBO ZOIMBA: 35, 62
July 7-13, 2008
TSAMBA 7
NYIMBO ZOIMBA: 95, 145
July 14-20, 2008
Chipulumutso Kudzera mu Ufumu wa Mulungu Chayandikira!
TSAMBA 12
NYIMBO ZOIMBA: 181, 130
July 21-27, 2008
Sankhani Kutumikira Yehova Mudakali Achinyamata
TSAMBA 17
NYIMBO ZOIMBA: 157, 221
July 28, 2008–August 3, 2008
Pitani Patsogolo Mwauzimu Potsanzira Paulo
TSAMBA 21
NYIMBO ZOIMBA: 123, 129
Cholinga cha Nkhani Zophunzira
Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 3-11
Paulaliki wake wotchuka wapaphiri, Yesu anatsindika kufunika kokhala ofatsa, achifundo ndi odzetsa mtendere. Analimbikitsa otsatira ake ‘kuonetsa kuwala kwawo,’ ndipo iye anafotokoza zimene tiyenera kuchitira adani athu ndiponso anthu ena.
Nkhani Yophunzira 3 MASAMBA 12-16
Dziwani mmene mungafotokozere chifukwa chimene tikufunikira kwambiri chipulumutso panopa kuposa kale lonse. Onani chifukwa chake Yehova ali Mpulumutsi Wamkulu ndi mmene mungasonyezere ena kuti Ufumu wa Mulungu upulumutsa anthu posachedwapa.
Nkhani Zophunzira 4, 5 MASAMBA 17-25
N’chifukwa chiyani achinyamata ayenera kutumikira Mulungu? Kodi iwo zingawayendere bwino atadzipereka kwa Yehova, ngakhale anthu aziwaona bwanji? Kodi iwo angachite utumiki wotani? Kodi chitsanzo cha mtumwi Paulo chingatithandize bwanji tonse mumpingo kupita patsogolo mwauzimu? Nkhani ziwirizi zikuyankha mafunso ofunika kwambiri amenewa.
M’MAGAZINI INO MULINSO:
TSAMBA 26
Mmene Bungwe Lolamulira Limayendetsera Ntchito Zake
TSAMBA 29
Mawu a Yehova Ndi Amoyo—Mfundo Zazikulu za M’buku la Machitidwe
TSAMBA 30