Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

September 15, 2008

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

November 3-9, 2008

Yehova ‘Anapulumutsa’ Anthu Ake M’nthawi za m’Baibulo

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 74, 44

November 10-16, 2008

Yehova Ndi “Mpulumutsi” Wathu

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 153, 3

November 17-23, 2008

Khalanibe ndi “Chingwe cha Nkhosi Zitatu” M’banja Lanu

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 117, 173

November 24-30, 2008

Pewani “Mzimu wa Dziko”

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 10, 191

Cholinga Cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 3-11

Nkhanizi zachokera pa Salmo 70. Pamenepo timapezapo mawu akuti Yehova ndi “mpulumutsi.” Nkhanizi zikufotokoza mmene Yehova anapulumutsira atumiki ake m’nthawi za m’Baibulo ndiponso mmene amatipulumutsira masiku ano.

Nkhani Yophunzira 3 MASAMBA 16-20

Masiku ano n’zovuta kuti anthu okwatirana akhale ogwirizana, ngakhale anthuwo atakhala atumiki a Yehova. M’nkhaniyi muli mfundo zothandiza zimene Akhristu angatsatire kuti Yehova akhale m’banja lawo, komanso zimene angachite pakakhala mavuto.

Nkhani Yophunzira 4 MASAMBA 20-24

Timafunika kusankha pakati pa zinthu ziwiri izi: Kutsogoleredwa ndi mzimu woyera wa Mulungu kapena ndi mzimu wa dzikoli. Nkhaniyi ikufotokoza zimene tingachite kuti mzimu wa Mulungu uzititsogolera komanso mmene tingapewere mzimu wa dziko. Ndipo itithandizanso kusankha zinthu zimene zingatipangitse kukhala osangalala.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Wonjezerani Chidwi Chofuna Kudziwa Zinthu Molondola

TSAMBA 12

Kulalikira Pamsika

TSAMBA 25

Tsanzirani Yesu​—Lambirani Mulungu Moyenera

TSAMBA 26

Mawu a Yehova Ndi Amoyo​—Mfundo Zazikulu za M’makalata Opita kwa Atesalonika ndi Timoteyo

TSAMBA 29

Mafunso Ochokera kwa Owerenga

TSAMBA 32