Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

October 15, 2008

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

December 1-7, 2008

“Maso Onyezimira” a Yehova Amasanthula Anthu Onse

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 160, 34

December 8-14, 2008

Yehova Amatiyang’ana ndi Zolinga Zabwino

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 81, 80

December 15-21, 2008

Mmene Yehova Akuyankhira Pemphero Lochokera Pansi Pamtima

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 74, 90

December 22-28, 2008

Kodi Mumakhala Patsogolo Posonyeza Ulemu?

TSAMBA 21

NYIMBO ZOIMBA: 216, 155

December 29, 2008–January 4, 2009

Kodi Mungalolere Kudzimana Chiyani Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha?

TSAMBA 25

NYIMBO ZOIMBA: 177, 212

Cholinga Cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 3-11

Nkhani ziwiri zimenezi zikutitsimikizira kuti Yehova amadziwa zonse zimene zimatichitikira. Amaona kupirira kwathu komanso amadziwa mavuto athu. Amaona kulimbikira kwathu konse komanso zimene zimachitikira atumiki ake. Kudziwa zimenezi n’kolimbikitsa.

Nkhani Yophunzira 3 MASAMBA 12-16

Ambirife timadziwa mawu a pa Salmo 83:18. Nanga bwanji za salmo lonselo? Nkhani imeneyi ikusonyeza kuti Salmo 83 lingalimbikitse kwambiri Akhristu masiku ano.

Nkhani Yophunzira 4 MASAMBA 21-25

Paulo ananena kuti: “Posonyezana ulemu wina ndi mnzake, khalani patsogolo.” Kodi kusonyeza ena ulemu kumatanthauza chiyani? Kodi ndani ayenera kusonyeza ulemu, nanga ndani ayenera kulemekezedwa? Kodi tili ndi zitsanzo zotani za m’Baibulo? Nkhani imeneyi ili ndi mfundo zothandiza.

Nkhani Yophunzira 5 MASAMBA 25-29

Tsiku lina Yesu anafunsa kuti: “Kodi munthu angapereke chiyani chosinthanitsa ndi moyo wake?” Kodi mungayankhe bwanji funso limeneli? Kodi zochita zanu zimasonyeza kuti mumakonda kwambiri moyo wanu? Nkhaniyi ikuthandizani kuganizira mofatsa funso la Yesu lofunika kwambiri limeneli.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

“Ilitu Ndi Dzina Loyera Ndiponso Lalikulu la Mulungu”

TSAMBA 16

“Yehova Ndiye Mphamvu Yanga”

TSAMBA 17

Mawu a Yehova Ndi Amoyo​—Mfundo Zazikulu za M’makalata Opita kwa Tito, Filemoni ndi Aheberi

TSAMBA 30