Zamkatimu
Zamkatimu
December 15, 2008
Magazini Yophunzira
NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
February 2-8, 2009
N’chifukwa Chiyani Muyenera Kusunga Umphumphu?
TSAMBA 3
NYIMBO ZOIMBA: 10, 160
February 9-15, 2009
TSAMBA 7
NYIMBO ZOIMBA: 26, 29
February 16-22, 2009
Udindo Wapadera wa Yesu Pokwaniritsa Cholinga cha Mulungu
TSAMBA 12
NYIMBO ZOIMBA: 205, 105
February 23, 2009–March 1, 2009
TSAMBA 16
NYIMBO ZOIMBA: 6, 193
Cholinga cha Nkhani Zophunzira
Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 3-11
Kodi umphumphu ndi chiyani? N’chifukwa chiyani kusunga umphumphu kuli kofunika? Kodi tingatani kuti tiyambe komanso tipitirizebe kusunga umphumphu? Kodi n’zotheka kuti munthu amene waswa umphumphu ayambirenso kuusunga? Nkhani ziwirizi zitithandiza kupeza mayankho a mafunso amenewa.
Nkhani Yophunzira 3 MASAMBA 12-16
Yesu ali ndi udindo wapadera pokwaniritsa cholinga cha Mulungu. Nkhaniyi ikufotokoza bwino mayina audindo 6 amene Yesu ali nawo. Mayina amenewa akusonyeza kuti Yesu ndi wapadera. Tionanso mmene Yesu wakwaniritsira udindo wake wapadera, ndiponso mmene tingamutsanzirire.
Nkhani Yophunzira 4 MASAMBA 16-20
Kukambirana zimene mtumwi Paulo anauza akulu a ku Efeso, zomwe zalembedwa m’chaputala 20 cha buku la Machitidwe, kutithandiza kudziwa zimene zinamuthandiza kuchitira umboni bwino lomwe. Tiphunziranso mmene tingachitire umboni bwino lomwe za uthenga wabwino komanso chifukwa chake tiyenera kuchita zimenezo.
M’MAGAZINI INO MULINSO:
Zolemba Zakale Zimatsimikizira Kuti Baibulo N’lolondola
TSAMBA 21
Ndaona Mboni za Yehova Zikuwonjezereka ku Korea
TSAMBA 23
Mawu a Yehova Ndi Amoyo—Mfundo Zazikulu za M’makalata a Yohane ndi Yuda
TSAMBA 27
TSAMBA 30
Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2008
TSAMBA 31
TSAMBA 32