Zamkatimu
Zamkatimu
March 15, 2009
Magazini Yophunzira
NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
May 4-10, 2009
TSAMBA 11
NYIMBO ZOIMBA: 222, 15
May 11-17, 2009
TSAMBA 15
NYIMBO ZOIMBA: 199, 129
May 18-24, 2009
Yehova Ndi Woyenera Kutamandidwa ndi Tonsefe
TSAMBA 20
NYIMBO ZOIMBA: 136, 169
May 25-31, 2009
Olungama Adzatamanda Mulungu Kosatha
TSAMBA 24
NYIMBO ZOIMBA: 48, 165
Cholinga Cha Nkhani Zophunzira
Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 11-19
Nkhani ziwirizi zikutikumbutsa kufunika koyang’anabe pa mphoto imene Mulungu watisungira. Kuphunzira za zinthu zoopsa zimene zichitike posachedwapa kutilimbikitsa kukhalabe maso.
Nkhani Zophunzira 3, 4 MASAMBA 20-28
Nkhani zimenezi zikufotokoza mwatsatanetsatane Masalmo 111 ndi 112, omwe ndi ogwirizana. Salmo 111 likutamanda Yehova chifukwa cha ntchito zake zodabwitsa komanso makhalidwe ake. Salmo 112 likusonyeza mmene ntchito zazikulu za Yehova ziyenera kutithandizira kuopa kumukhumudwitsa komanso kutilimbikitsa kutengera makhalidwe ake apamwamba.
M’MAGAZINI INO MULINSO:
“Mngelo wa Yehova Azinga” Anthu Ake
TSAMBA 3
TSAMBA 6
Kodi N’chiyani Chingakuthandizeni Kupirira Muutumiki?
TSAMBA 29
TSAMBA 32