Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Zamkatimu

Zamkatimu

Zamkatimu

March 15, 2009

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

May 4-10, 2009

Yang’ananibe pa Mphoto

TSAMBA 11

NYIMBO ZOIMBA: 222, 15

May 11-17, 2009

“Khalani Maso”

TSAMBA 15

NYIMBO ZOIMBA: 199, 129

May 18-24, 2009

Yehova Ndi Woyenera Kutamandidwa ndi Tonsefe

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 136, 169

May 25-31, 2009

Olungama Adzatamanda Mulungu Kosatha

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 48, 165

Cholinga Cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 11-19

Nkhani ziwirizi zikutikumbutsa kufunika koyang’anabe pa mphoto imene Mulungu watisungira. Kuphunzira za zinthu zoopsa zimene zichitike posachedwapa kutilimbikitsa kukhalabe maso.

Nkhani Zophunzira 3, 4 MASAMBA 20-28

Nkhani zimenezi zikufotokoza mwatsatanetsatane Masalmo 111 ndi 112, omwe ndi ogwirizana. Salmo 111 likutamanda Yehova chifukwa cha ntchito zake zodabwitsa komanso makhalidwe ake. Salmo 112 likusonyeza mmene ntchito zazikulu za Yehova ziyenera kutithandizira kuopa kumukhumudwitsa komanso kutilimbikitsa kutengera makhalidwe ake apamwamba.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

“Mngelo wa Yehova Azinga” Anthu Ake

TSAMBA 3

Musaiwale Yehova

TSAMBA 6

Kodi N’chiyani Chingakuthandizeni Kupirira Muutumiki?

TSAMBA 29

Mafunso Ochokera kwa Owerenga

TSAMBA 32