Zamkatimu
Zamkatimu
November 15, 2009
Magazini Yophunzira
NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
December 28, 2009–January 3, 2010
Kodi Mapemphero Anu Amasonyeza Chiyani za Inuyo?
TSAMBA 3
NYIMBO ZOIMBA: 51, 13
January 4-10, 2010
Kuphunzira Baibulo Kungathandize Kuti Mapemphero Anu Azikhala Atanthauzo
TSAMBA 7
NYIMBO ZOIMBA: 6, 22
January 11-17, 2010
Yamikirani Malo Anu Mumpingo wa Mulungu
TSAMBA 13
NYIMBO ZOIMBA: 53, 48
January 18-24, 2010
Pitirizani Kukulitsa Chikondi Chanu Chaubale
TSAMBA 20
NYIMBO ZOIMBA: 25, 50
January 25-31, 2010
Tiyenera Kukhala Aulemu Popeza Ndife Atumiki a Mulungu
TSAMBA 24
NYIMBO ZOIMBA: 34, 3
Cholinga cha Nkhani Zophunzira
Nkhani Zophunzira 1 ndi 2 TSAMBA 3-11
Pa nkhani ziwirizi, yoyamba ikuthandizani kuonanso bwino mapemphero anu kwa Yehova. Yachiwiri ikulimbikitsani kuti muziwerenga bwinobwino mapemphero ndiponso mawu otamanda ndi kuyamika Mulungu amene analembedwa m’Baibulo, ndipo kuchita zimenezi kungakuthandizeni kudziwa zimene mungachite kuti mapemphero anu azikhala atanthauzo.
Nkhani Yophunzira 3 TSAMBA 13-17
Mkhristu aliyense ali ndi malo ake mumpingo wa Yehova. Nkhaniyi ikufotokoza njira zosiyanasiyana zimene tingasonyezere kuti timayamikira malo athu mumpingo wachikhristu.
Nkhani Zophunzira 4, 5 TSAMBA 20-29
Kusonyeza chikondi chaubale n’kofunika kwambiri kuti mumpingo mukhale mgwirizano. Ndipo ulemu ndi wofunika kwambiri mu utumiki wakumunda. Nkhanizi zikusonyeza mmene tingakulitsire makhalidwe awiriwa pa moyo wathu.
M’MAGAZINI INO MULINSO:
TSAMBA 12
Kupereka Mokondwera Kuchokera Pansi pa Mtima
TSAMBA 18
TSAMBA 29
Muziona Kuti Abale ndi Alongo Anu Osamva Ndi Ofunika Kwambiri
TSAMBA 30