Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2011

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2011

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2011

Wosonyeza deti la magazini imene muli nkhaniyo

BAIBULO

Kodi Mumasangalala Kuwerenga? 5/15

Kodi Nthawi Ankaitchula Bwanji? 5/1

Limasintha Anthu, 2/1, 4/1, 5/1, 7/1, 8/1, 10/1, 11/1

Linalembedwa Liti, 6/1

Maulosi 6 a M’Baibulo Amene Akukwaniritsidwa, 5/1

Olivétan​—‘Anamasulira,’ 9/1

Pa Anthu Olemba Malemba Achigiriki, ndi Ati Amene Analipo pa Pentekosite? 12/1

Zamora Anayesetsa Kumasulira Molondola, 12/1

Zoti Achinyamata Achite, 1/1, 3/1, 5/1, 7/1, 9/1, 11/1

MBIRI YA MOYO WANGA

Kutumikira Yehova Kwandibweretsera Chimwemwe (F. Rusk), 10/15

Kutumikira Yehova Ngakhale pa Nthawi Zovuta (M. de Jonge-van den Heuvel), 1/15

Kuwerenga Baibulo Kwandilimbikitsa pa Moyo Wanga Wonse (M. Leroy), 9/15

Ndapeza Zinthu Zambiri Zabwino (A. Bonno), 4/15

Ndapindula Kwambiri Chifukwa Chololera Kusintha Zinthu (J. Thompson), 12/15

Ndinkafunitsitsa Ntchito Yoyenda M’madera Osiyanasiyana (Z. Dimitrova), 6/1

Ndinkaopa Imfa Koma Tsopano Ndikuyembekezera ‘Moyo Wochuluka’ (P. Gatti), 7/15

Ngati Mwana wa Yefita (J. Soans), 12/1

“Panopa Ndine Wolumala, Koma Sindidzakhala Chonchi Mpaka Kalekale” (S. van der Monde), 11/15

“Woyang’anira Wabwino Ndiponso Mnzathu Wapamtima” (J. Barr), 5/15

MBONI ZA YEHOVA

“Anthu Olimba Mtima Ofunika Kuwayamikira” (Germany), 10/1

Kalata Yochokera ku . . . , 3/1, 6/1, 9/1, 12/1

Kodi Amalandira Chithandizo Chachipatala? 2/1

Kuwina Milandu Imene Yatenga Nthawi Yaitali (Russia), 7/15

Kuyesetsa Kuti Anthu Asaipitse Mbiri Yawo (Russia), 5/1

Misonkhano Yachigawo ku Russia, 3/1

Misonkhano Yachigawo yakuti, “Ufumu wa Mulungu Ubwere,” 6/1

Msonkhano Wapachaka, 8/15

Mwambo Womaliza Maphunziro a Giliyadi, 2/1, 8/1

“Mwayi Wopereka Nawo Mphatso Zachifundo” (zopereka), 11/15

Nsanja ya Olonda ya M’Chingelezi Chosavuta, 7/15

Zinthu Zimene Mungakondwere Nazo (gulu la Mulungu), 3/15

Ziwerengero za mu Lipoti la Chaka Chautumiki, 8/15

MOYO NDI MAKHALIDWE ACHIKHRISTU

Abambo Azigwirizana ndi Ana Awo Aamuna, 11/1

Banja Lanu Lizikonda Zinthu Zauzimu, 11/1

Funso Kapena Ngati Ndili ndi Vuto, 10/15

Khalani Olimba Mtima Ngati Pinihasi, 9/15

Khalanibe Oona Mtima M’dziko la Anthu Osaona Mtima, 4/15

Kodi Achinyamata Ayenera Kubatizidwa? 6/15

Kodi Makolo Aziphunzitsa Ana Awo Nkhani Zokhudza Kugonana? 11/1

Kodi Mumayamikira Madalitso Amene Muli Nawo? 2/15

Kugwiritsa Ntchito Intaneti, 8/15

Kukhala ndi “Moyo Wopambana,” 6/15

‘Kukhalabe Maso,’ 10/15

Kulambira kwa Pabanja, 8/15

“Kumvera Kuposa Nsembe,” 2/15

Misonkho, 9/1

Mungatani Kuti Banja Lanu Likhale Lolimba? 2/1

Mungatani Kuti Banja Lanu Likhale Losangalala? 10/1

Musadzinyenge ndi Maganizo Onama, 3/15

Musalole Kuti Matenda Akulandeni Chimwemwe, 12/15

Musasiye Okhulupirira Anzanu, 3/15

Muziganizira Zimene Yehova Wakuchitirani Kale, 1/15

Muzilemekeza Mwamuna Kapena Mkazi Wanu, 8/1

Muziphunzitsa Ana Anu Makhalidwe Abwino, 2/1

‘Nthawi ya Chikondi, Nthawi ya Chidani,’ 12/1

Phunzitsani Ana Anu, 2/1, 4/1, 6/1, 8/1, 10/1, 12/1

Phunzitsani Ana Anu Ulemu, 2/15

Tingapeze Bwanji Anzathu Abwino? 12/1

Tiyenera Kuchita Khama (Kulambira kwa Pabanja), 2/15

Tiyeni Tisangalale Limodzi, 10/15

Umboni Wakuti Mulungu Akutitsogolera, 4/15

Zinthu Zimasintha M’banja Mukabadwa Mwana, 5/1

NKHANI ZOPHUNZIRA

Anapeza Mesiya, 8/15

Anthu Amene Amakhulupirira Yehova Amakhala Olimba Mtima, 5/15

Anthu Ankayembekezera Mesiya, 8/15

Anthu Okhulupirika Akale Amene Anatsogoleredwa ndi Mzimu wa Mulungu, 12/15

Anthu Ovomerezeka ndi Mulungu Adzapeza Moyo Wosatha, 2/15

Khalani Okonzeka, 3/15

Khalani Tcheru Ngati Yeremiya, 3/15

Khulupirirani Yehova, “Mulungu Amene Amatitonthoza M’njira Iliyonse,” 10/15

Kodi Mpumulo wa Mulungu N’chiyani? 7/15

Kodi Mukulola Mzimu wa Mulungu Kukutsogolerani? 4/15

Kodi Mukulola Yehova Kukhala Cholowa Chanu? 9/15

Kodi Mukutsatira Machenjezo a Yehova Omveka Bwino? 7/15

Kodi Mukutsatira Malangizo Achikondi a Yehova? 7/15

Kodi Mumadana Ndi Kusamvera Malamulo? 2/15

Kodi Mumadziwika ndi Yehova? 9/15

Kodi Munthu Wofunika Kwambiri pa Moyo Wanu Ndi Ndani? 5/15

Kodi Mwalowa mu Mpumulo wa Mulungu? 7/15

Kodi Solomo Ndi Chitsanzo Chabwino Kapena Choipa? 12/15

Kodi Zimene Mumachita pa Nthawi Yosangalala Zimakhala Zopindulitsa? 10/15

Landirani Mzimu wa Mulungu Osati wa Dziko, 3/15

Mabanja Achikhristu Ayenera ‘Kukhala Okonzeka,’ 5/15

Mabanja Achikhristu Ayenera ‘Kukhalabe Maso,’ 5/15

“Makhalidwe Amene Mzimu Woyera Umatulutsa” Amalemekeza Mulungu, 4/15

Malangizo Anzeru kwa Anthu Amene Sali Pabanja Ndiponso Amene Ali Pabanja, 10/15

Mulungu Akuonetsa Chikondi Chake kwa Ife, 6/15

Muzidalira Yehova Pamene Mapeto Akuyandikira, 3/15

Muzigwiritsa Ntchito Mwanzeru Nthawi Imene Simuli pa Banja, 1/15

Muzikonda Chilungamo ndi Mtima Wanu Wonse, 2/15

“Muzilemekeza Anthu Amene Akugwira Ntchito Mwakhama Pakati Panu,” 6/15

Muzilemekeza Ukwati Monga Mphatso Yochokera kwa Mulungu, 1/15

Mzimu wa Mulungu Unkatsogolera Akhristu Oyambirira Ndipo Ukutsogoleranso Akhristu Masiku Ano, 12/15

Mzimu Woyera Umatipatsa Mphamvu Yolimbana ndi Mayesero Ndiponso Zofooketsa, 1/15

Mzimu Woyera Umatipatsa Mphamvu Yolimbana ndi Vuto Lililonse, 1/15

Mzimu Woyera Unagwira Ntchito Polenga Zinthu, 2/15

N’chifukwa Chiyani Tiyenera kutsogoleredwa ndi Mzimu wa Mulungu? 12/15

Ndife “Osakhalitsa” M’dziko Loipali, 11/15

‘Nzeru za Mulungu N’zozama’ Kwambiri (Aroma 11), 5/15

Pali Uthenga Wabwino Wofunika Kuti Anthu Onse Amve, 6/15

‘Pezani Chitetezo M’dzina la Yehova,’ 1/15

‘Thamangani N’cholinga Choti Mukalandire Mphoto,’ 9/15

Thandizani Amuna Kukula Mwauzimu, 11/15

Thandizani Ena Kuti Ayenerere Maudindo, 11/15

Tiyeni Tithamange Mpikisano Mopirira, 9/15

Tiziona Kuti Kutumikira Yehova Ndi Chinthu Chofunika Kwambiri, 4/15

‘Tonthozani Anthu Onse Olira,’ 10/15

“Usadalire Luso Lako Lomvetsa Zinthu,” 11/15

“Wetani Gulu la Nkhosa za Mulungu Lomwe Analisiya M’manja Mwanu,” 6/15

Yehova Ndi Cholowa Changa, 9/15

Yehova Ndi “Mulungu Amene Amapatsa Mtendere,” 8/15

Yendani Mogwirizana ndi Mzimu Kuti Mupeze Moyo ndi Mtendere, 11/15

Yesetsani Kukhala pa Mtendere ndi Ena, 8/15

Zosankha Zanu Zizilemekeza Mulungu, 4/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

“A M’nyumba ya Kaisara” (Afil. 4:22), 3/1

“Akazi Ambiri” (Mlal. 2:8), 3/15

Anakhalabe Wokhulupirika Ngakhale Anakumana ndi Mavuto (Samueli), 1/1

Analimba Mtima Kuteteza Anthu a Mulungu (Esitere), 10/1

Analimbikitsidwa ndi Mulungu (Eliya), 7/1

Anthu Osintha Ndalama M’kachisi, 10/1

Atumwi Anatenga Ndodo N’kuvala Nsapato, 3/15

Baraba, 4/1

“Chikondwerero cha kupereka kachisi kwa Mulungu” (Yohane 10:22), 9/1

“Dziko Loyenda Mkaka ndi Uchi,” 3/1

Kodi Abulahamu Analidi ndi Ngamila? 6/15

Kodi Akhristu Onse Okhulupirika Amapita Kumwamba? 6/1

Kodi Akufa Adzauka? 6/1

Kodi Amene Akulamulira Dzikoli Ndani? 9/1

Kodi Aramagedo N’chiyani? 9/1

Kodi Atsogoleri Achipembedzo Achiyuda Ankawaona Bwanji Anthu Wamba? 7/1

Kodi Chipembedzo Choona Mungachidziwe bwanji? 8/1

Kodi Dzikoli Litha mu 2012? 12/1

Kodi Gehena Ndi Malo Amene Anthu Amakapsa? 4/1

Kodi Masoka Achilengedwe Ndi Chilango? 12/1

Kodi Moyo Wosatha Udzafika Potopetsa? 5/1

Kodi Mukukonzekera Tsiku Lofunika Kwambiri? 2/1

Kodi Munthu Ankaphedwa Ngati Yesu Akapalamula Mlandu Wotani? 4/1

Kodi N’chifukwa Chiyani Satana Anagwiritsa Ntchito Njoka? 1/1

Kodi N’chifukwa Chiyani Solomo Anaitanitsa Mitengo ku Lebanoni? 2/1

Kodi Ndani Angamasulire Ulosi? 12/1

Kodi Papa Ndi Wolowa M’malo mwa Petulo? 8/1

Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani? 7/1

Kodi Ufumu wa Mulungu Uli Mumtima? 3/1

Kodi Yerusalemu Anawonongedwa Liti? 10/1, 11/1

Kubatiza Ana Akhanda, 10/1

Kudziwa Nthawi Usiku, 8/1

Kugula Zinthu Mogwirizana ndi Ndalama, 6/1

‘Kumenya Zisonga Zotosera’ (Mac. 26:14), 8/1

Kupeza Madzi M’nyengo ya Chilimwe ku Isiraeli, 1/1

Kutchova Juga, 3/1

Kuthetsa Umphawi, 6/1

Lamulo Lokhudza Khunkha, 2/1

Mayina Odindidwa pa Zomatira Zadongo, 5/1

Mitengo ya Maolivi Ankaiona Kuti Ndi Yofunika , 10/1

“Mitundu 7 ya Mbewu” M’dziko Labwino, 9/1

Moyo Waphindu, 7/1

Munda wa Edeni, 1/1

Munthu wa Kum’mawa kwa Asia Anapezeka ku Italy, 1/1

Munthu Wapamtima pa Yehova, 9/1

N’chifukwa Chiyani Mose Anakwiyira Ana a Aroni? (Lev. 10:16-20), 2/15

Ndalama (Moyo wa anthu akale), 5/1

Ndalama Zoyendetsera Ntchito Zapakachisi, 11/1

“Ndimakhulupirira” (Malita), 4/1

Nyumba Imene Abulamu Ankakhala, 1/1

Petulo Anali Kunyumba ya Wofufuta Zikopa, 6/1

Tanthauzo la dzina loti Kaisara, 7/1

Ukwati Wapachilamu Kapena Kuti Wolowa Chokolo, 3/1

“Ulusi Wofiira Kwambiri,” 12/1

‘Unditengerenso Mipukutu Makamaka Yazikopa,’ 6/15

‘Uthenga Wabwino wa Ufumu,’ 3/1

Yehu Anamenyera Nkhondo Kulambira Koyera, 11/15

Zimene Baibulo Limanena pa Nkhani ya Kugonana, 11/1

Zinthu Zimene Nebukadinezara Anamanga, 11/1

YEHOVA

Dzina lake M’chigwa (Switzerland), 1/15

Kodi Ali ndi Gulu Lake? 6/1

Kodi Ali ndi Malo Enieni Amene Amakhala? 8/1

Kodi Amakukondanidi? 1/1

Kodi Amaona Kuti Mtundu Wina Ndi Wofunika? 7/1

Kodi Ana Ayenera Kuphunzitsidwa Chiyani? 8/1

Kodi Anadziwiratu Kuti Adamu ndi Hava Adzachimwa? 1/1

Kodi Analenga Mdyerekezi? 3/1

Kodi Analengeranji Dziko Lapansi? 4/1

Kodi Mulungu Ndani? 2/1

Malamulo a Zinthu Zakuthambo, 7/1

Malamulo Ake Amatithandiza, 11/1

N’Chifukwa Chiyani Ankapatsa Aisiraeli Zinziri? 9/1

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzitsidwa Naye? 1/1

N’chifukwa Chiyani Walola Kuti Zoipa Zizichitika? 5/1

Yandikirani Mulungu, 1/1, 2/1, 3/1, 4/1, 5/1, 6/1, 7/1, 8/1, 9/1, 10/1, 11/1, 12/1

Zikhulupiriro Zisanu Zabodza, 10/1

YESU KHRISTU

Anaweruzidwa Mopanda Chilungamo, 4/1

Chiwerengero cha Maulosi Onena za Mesiya, 8/15

Kodi Anachokera Kuti; Anachita Zotani; N’chifukwa Chiyani Anafa? 4/1

Kodi Anafera Pamtanda? 3/1

Kodi Yesu Khristu Ndani? 3/1

Mawu akuti “Mwanena Nokha,” 6/1

Nthawi Imene Anapachikidwa, 11/15

Tsatirani Khristu Yemwe Ndi Mtsogoleri Wabwino Kwambiri, 5/15