Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2012

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2012

Wosonyeza deti la magazini imene muli nkhaniyo

BAIBULO

  • Baibulo la Chingelezi la Coverdale, 6/1

  • Kodi Limalosera Zam’tsogolo? 1/1

  • Kuligwiritsa Ntchito Ngati Chithumwa, 12/15

  • La Chiswahili, 9/1

  • Limasintha Anthu, 1/1, 2/1, 4/1, 5/1, 7/1, 8/1, 10/1, 11/1

  • N’losiyana ndi Mabuku Ena, 6/1

  • Zoti Achinyamata Achite, 1/1, 4/1, 7/1, 10/1

MBIRI YA MOYO WANGA

  • “Chinsinsi” Chimene Taphunzira Potumikira Mulungu (O. Randriamora), 6/15

  • “Kudzanja Lamanja Kuli Chimwemwe” (L. Didur), 3/15

  • Mawu a Mulungu Anathandiza Banja Lachihindu (N. Govindsamy), 10/1

  • Ndagwira Chovala cha Myuda kwa Zaka 70 (L. Smith), 4/15

  • Ndinapeza Ufulu Weniweni (M. Kilin), 12/1

  • Ndinkacheza ndi Achikulire Anzeru (E. Gjerde), 5/15

  • Tsopano Ndikudziwa Mulungu Amene Ndikum’tumikira (M. Bacudio), 9/1

  • Ubwenzi wa Zaka 60 (L. Turner, W. Kasten, R. Kelsey, R. Templeton), 10/15

  • Yehova Anandiphunzitsa Kuchita Chifuniro Chake (M. Lloyd), 7/15

  • Yehova Watsegula Maso Anga (P. Oyeka), 6/1

MBONI ZA YEHOVA

  • Aaziteki, 3/1

  • Akopotala, 5/15

  • Anadzipereka ku Brazil, 10/15

  • Anadzipereka ku Ecuador, 7/15

  • ‘Anali Asanamvepo Uthenga Wabwino’ (wailesi ku Canada), 11/15

  • Ankalalikira Mawu a Mulungu Molimba Mtima, 2/15

  • Kalata Yochokera . . . , 3/1, 6/1, 9/1, 12/1

  • ‘Kankachititsa Kuti Ndizionekera Patali’ (kanjinga), 2/15

  • Khoti Linagamula za Ufulu Wokana Usilikali (V. Bayatyan), 11/1

  • Kodi Akazi Amaphunzitsa Mawu a Mulungu? 9/1

  • “Kodi Mungatijambule?” (Mexico), 3/15

  • ‘Kodi Ndingakwanitse Kulalikira?’ (wolumala), 1/15

  • Kukomera Mtima Munthu Wokwiya Kumathandiza, 6/15

  • Kusunga Zinthu Zathu Zamtengo Wapatali, 1/15

  • Magazini Yophunzira (Nsanja ya Olonda), 1/15

  • Mawu a “Ana Aang’ono” (Russia, Australia), 10/15

  • Misonkhano Yachigawo Yakuti ‘Tetezani Mtima Wanu,’ 5/1

  • Msonkhano Wapachaka, 8/15

  • Mwambo wa Omaliza Sukulu ya Giliyadi, 2/1, 8/1

  • N’chifukwa Chiyani Timalalikira Kunyumba ndi Nyumba? 6/1

  • Nsanja ya Olonda ya M’Chingelezi Chosavuta, 12/15

  • Ogwirizana M’mayiko Osiyana (Portugal, Spain, France), 1/1

  • Oyang’anira Oyendayenda Akale, 8/15

  • Sukulu Zophunzitsa Atumiki a Mulungu, 9/15

  • “Zimene Ndinkafuna Zatheka” (upainiya), 7/15

  • Zimene Zinachitika ku Estonia, 12/1

  • Zochuluka Zinathandiza Osowa (zopereka), 11/15

MOYO NDI MAKHALIDWE ACHIKHRISTU

  • Chikalata Cholumbira Kukhulupirika mu Ukwati, 12/15

  • Kodi Akhristu a M’nthawi ya Atumwi Ankachita Nawo Ndale? 5/1

  • Kodi Banja Limapangitsa Munthu Kukhala Wosangalala? 10/1

  • Kodi Mkhristu Angachotsedwe Chifukwa Choonera Zolaula? 3/15

  • Kodi Mumatani Ena Akakupemphani Malangizo? 3/15

  • Kukoma Mtima, 9/1

  • Kupindula ndi Kusangalala Mukamaphunzira, 1/15

  • Mphatso Yokhala Wosakwatira, 11/15

  • Muzifufuza “Nzeru Zoyendetsera Moyo,” 6/15

  • Mwana Wanu Akayamba Kukayikira Chipembedzo, 2/1

  • N’chifukwa Chiyani Akhristu Amabatizidwa? 4/1

  • Ngongole, 11/1

  • Phunzitsani Ana Anu, 3/1, 6/1, 9/1, 12/1

  • “Samalani ndi Chofufumitsa cha Afarisi,” 5/15

  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo, 2/1, 5/1, 8/1, 11/1

NKHANI ZOPHUNZIRA

  • Akhristu Oona Amalemekeza Mawu a Mulungu, 1/15

  • ‘Anatsogoleredwa ndi Mzimu Woyera,” 6/15

  • Ansembe Achifumu Amene Adzapindulitse Anthu Onse, 1/15

  • “Anthu Osakhalitsa M’dzikoli” Ndi Ogwirizana Polambira Mulungu, 12/15

  • “Ine Ndili Pamodzi ndi Inu,” 8/15

  • ‘Khalani Olimba Mtima Kwambiri Ndipo Muchite Zinthu Mwamphamvu,’ 2/15

  • Khalanibe Odzipereka, 3/15

  • Khulupirirani Yehova, Mulungu wa “Nthawi ndi Nyengo,” 5/15

  • Kodi Dzikoli Lidzatha Bwanji? 9/15

  • Kodi Mukuonetsa Ulemerero wa Yehova? 5/15

  • Kodi Mumaika Kutumikira Yehova pa Malo Oyamba? 6/15

  • Kodi Mumaonetsa Mzimu Wotani? 10/15

  • Kusakhulupirika Ndi Chizindikiro cha Masiku Otsiriza, 4/15

  • Limbani Mtima Pokumana ndi Mavuto, 10/15

  • Lolani Yehova Kukutsogolerani ku Ufulu Weniweni, 7/15

  • Mtendere Udzayamba mu Ulamuliro wa Zaka 1,000, 9/15

  • Mukati Inde Akhaledi Inde, 10/15

  • Mukhoza Kukhala ndi Moyo Wabwino Kwambiri, 12/15

  • Musamayang’ane “Zinthu za M’mbuyo,” 3/15

  • Musasunthike Popewa Misampha ya Satana, 8/15

  • Musataye Mtima Ngati Banja Lanu Silikuyenda Bwino, 5/15

  • Muzichita Zinthu Monga Nzika za Ufumu, 8/15

  • Muzikhululukirana ndi Mtima Wonse, 11/15

  • Muziyamikira Mphatso ya Ukwati Yochokera kwa Mulungu, 5/15

  • Mverani Mulungu Kuti Mupindule ndi Malumbiro Ake, 10/15

  • ‘Mwana Amakonda Kuululira Ena za Atate,’ 4/15

  • “Ndingachitenso Mantha ndi Ndani?” 7/15

  • Ndinu Mtumiki Wokhulupirika, 12/15

  • “Ndiphunzitseni Kuchita Chifuniro Chanu,” 11/15

  • N’zotheka Kukhala Osangalala M’banja Limene Wina Si Mboni, 2/15

  • Phunzirani Kuchokera ku Choonadi cha M’chilamulo, 1/15

  • Phunzirani Kukhala Maso Kuchokera kwa Atumwi a Yesu, 1/15

  • Pitirizani Kukhala Monga “Anthu Osakhalitsa M’dzikoli,” 12/15

  • Pitirizani Kutumikira Yehova ndi Mtima Wathunthu, 4/15

  • Samalani ndi Misampha ya Mdyerekezi, 8/15

  • “Simukudziwa Tsiku Kapena Ola Lake,” 9/15

  • Thandizani Anthu Kuti ‘Adzuke ku Tulo,’ 3/15

  • Thandizani Mpingo Kukhalabe ndi Maganizo Abwino, 2/15

  • Tizipereka Nsembe kwa Yehova ndi Moyo Wathu Wonse, 1/15

  • Tizisangalala ndi Chiyembekezo Chathu, 3/15

  • Tsanzirani Kuleza Mtima kwa Yehova ndi Yesu, 9/15

  • Tsanzirani Yesu pa Nkhani Yokhala Maso, 2/15

  • Tumikirani Mulungu Amene Amapereka Ufulu, 7/15

  • Yehova Akusonkhanitsa Banja Lake, 7/15

  • Yehova Amadziwa Kupulumutsa Anthu Ake, 4/15

  • Yehova Amasonkhanitsa Anthu Ake Osangalala, 9/15

  • Yehova Amatiteteza Kuti Tidzapulumuke, 4/15

  • Yehova Ndi Wofunitsitsa Kukukhululukirani, 11/15

  • Yehova Ndi “Woulula Zinsinsi,” 6/15

  • Yehova Waulula “Zimene Ziyenera Kuchitika Posachedwapa,” 6/15

  • Yesetsani Kukhala Ngati Wamng’ono, 11/15

  • Yesu Anatipatsa Chitsanzo cha Kudzichepetsa, 11/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

  • Abulahamu, 1/1

  • Ahasiwero (m’buku la Esitere), 1/1

  • Akhristu Anathawa mu Yudeya Chaka cha 70 C.E Chisanafike, 10/1

  • “Ana a Aneneri,” 10/1

  • Anachita Zinthu Mwanzeru, Molimba Mtima, Moganizira Ena (Esitere), 1/1

  • Anasi wa M’Mauthenga Abwino, 4/1

  • Ankateteza ndi Kusamalira Banja Lake (Yosefe), 4/1

  • Aramagedo, 2/1

  • Chipembedzo Ndiponso Ndale, 5/1

  • Fodya, 8/1

  • Guwa la “Mulungu Wosadziwika,” 3/1

  • Imfa ya Okhulupirika a Yehova “Ndi Nkhani Yaikulu,” 5/15

  • Inki ndi Zolembera Zakale, 11/1

  • Kaduka, 2/15

  • Kodi Abwino Amapita Kumwamba? 8/1

  • Kodi Anthu Ankaimba Zitoliro pa Maliro? 2/1

  • Kodi Anthu Ankatumiza Bwanji Makalata? 9/1

  • Kodi Dziko Lapansili Lidzawonongedwa? 2/1

  • Kodi Kukhala ndi Chikhulupiriro N’kusaganiza Bwino? 11/1

  • Kodi Mchere Umatha Mphamvu? (Mat. 5:13), 12/1

  • Kodi Mungawadziwe Bwanji Akhristu? 3/1

  • Kodi Musanabadwe Munakhalapo Kwinakwake? 12/1

  • Kodi N’zosathekadi? 6/1

  • Kodi N’zotheka Kukhala ndi Moyo Kwamuyaya? 10/1

  • Kodi Ziphuphu Zidzatha? 10/1

  • Kugwiritsa Ntchito Phula Ngati Matope, 7/1

  • Kugwiritsa Ntchito Vinyo Ngati Mankhwala, 8/1

  • Kukhulupirira Zamizimu, 3/1

  • “Kumene Inu Mupite Inenso Ndipita” (Rute), 7/1

  • Kupeza Ndalama Zochepa, 6/1

  • Kusunga M’firiji Mazira Amene Ayamba Kukula, 12/15

  • Kutaya Ndalama ya Dalakima, 12/1

  • Kuweruza Potengera Maonekedwe, 3/1

  • Kuyambiranso Kukhulupirirana (chigololo), 5/1

  • Mahema Omwe Mtumwi Paulo Ankapanga, 11/1

  • Mapepala pa Nthawi Imene Baibulo Linkalembedwa, 7/1

  • M’busa (anthu akale), 11/1

  • Mibadwo ya Makolo Achiyuda, 6/1

  • Miyala ya Pachovala cha Mkulu wa Ansembe, 8/1

  • “Mkazi Wabwino Kwambiri” (Rute), 10/1

  • Mlimi (anthu akale), 5/1

  • ‘Mpando Woweruzira Milandu’ (Mac. 18:12), 5/1

  • “Mphoto Chifukwa cha Ntchito Yanu” (Asa), 8/15

  • Msodzi (anthu akale), 8/1

  • Mungadzakhale ndi Tsogolo Labwino, 5/1

  • Natani Ankalimbikitsa Kulambira Koona, 2/15

  • N’chifukwa Chiyani Ena Sachita Khirisimasi? 12/1

  • N’chiyani Chidzachitikire Zipembedzo? 5/1

  • Njerwa ku Iguputo Wakale, 1/1

  • Nsalu Zakale Komanso Mitundu Yake, 3/1

  • Oimba Nyimbo Komanso Zida Zawo (anthu akale), 2/1

  • Okhometsa Misonkho (m’nthawi ya atumwi), 3/1

  • Pali Zosangalatsa Kuposa Khirisimasi, 12/1

  • Pamene Britain ndi America Anakhala Ulamuliro wa 7, 6/15

  • Sankayenera Kukwatirana ndi Anthu a Mitundu Ina, 7/1

  • Tesalonika, 6/1

  • Tsiku la Chiweruzo, 9/1

  • Utatu, 3/1

  • Yehova Anaulula Mafumu 8, 6/15

  • Zamalonda mu Isiraeli, 9/1

  • Zochita za Angelo ndi Ziwanda Zimatikhudza, 7/1

  • Zodzoladzola za Anthu Akale, 12/1

  • Zozizwitsa, 8/1

YEHOVA

  • Amamva Mapemphero, 7/1

  • Atate, 7/1

  • Kodi Adzakhazikitsa Boma Lolamulira Dziko Lonse? 11/1

  • Kodi Amalanga Anthu Kumoto? 10/1

  • Kodi Amaona Kuti Akazi Ndi Otsika? 9/1

  • Kodi Mungam’funse Chiyani? 11/1

  • N’chifukwa Chiyani Ali ndi Gulu? 2/1

  • N’chifukwa Chiyani Anatumiza Yesu Padziko? 12/1

  • N’chifukwa Chiyani Anauza Abulahamu Kupereka Mwana Wake? 1/1

  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kugwiritsa Ntchito Dzina Lake? 6/1

  • Yandikirani Mulungu, 1/1, 2/1, 3/1, 4/1, 5/1, 6/1, 7/1, 8/1, 9/1, 10/1, 11/1, 12/1

YESU KHRISTU

  • Ayuda Anakhumudwa ndi Mmene Yesu Anafera, 5/1

  • Kodi Anakhala Liti Mfumu? 8/1

  • Kodi Ankachita Nawo Ndale? 5/1

  • Kodi Tizikumbukira Bwanji Imfa ya Yesu? 3/1

  • Kodi Yesu Ndi Mulungu? 4/1

  • Mabuku Amene Ena Amati Ndi Mauthenga Abwino, 4/1

  • Mafunso Onena za Yesu, 4/1

  • Mlandu wa Amene Anapachikidwa Limodzi ndi Yesu, 2/1

  • Ndani Anatumiza Nyenyezi? 4/1

  • “Umunyamulire Mtunda wa Makilomita Awiri” (Mat. 5:41), 4/1