Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Tsamba 32

Tsamba 32

Tsamba 32

▪ Kodi n’chiyani chingakuthandizeni kukhala ndi mtendere wa mumtima ngakhale muli pa umphawi, mukudwala kapena mukuona kuti mukhoza kumwalira?

TSAMBA 9.

▪ Kodi kupemphera m’dzina la Yesu n’kofunika pa zifukwa zitatu ziti?

TSAMBA 13.

▪ N’chifukwa chiyani lilime tingaliyerekezere ndi moto?

TSAMBA 19.

▪ N’chifukwa chiyani Mulungu amalola kuti tizivutika?

TSAMBA 27.

▪ Kodi ndi mavuto ena ati amene azimayi omwe ali pantchito amakumana nawo kawirikawiri?

TSAMBA 28.