Tsamba 32
Tsamba 32
▪ Kodi dzina la Mulungu ndi ndani? Onani tsamba 6.
▪ Kodi ndani kwenikweni akulamulira dzikoli? Onani tsamba 8.
▪ Ngati muli ndi ana, kodi n’chifukwa chiyani ndi bwino kukhala ndi nthawi yocheza ndi mwamuna kapena mkazi wanu? Onani tsamba 11.
▪ Kodi mayi amene ankazembetsa miyala ya diamondi komanso kuwabera abwana ake anasintha bwanji kukhala woona mtima? Onani masamba 26 ndi 27.
▪ Kodi n’chifukwa chiyani Mboni za Yehova sizigwiritsa ntchito mafano polambira? Onani masamba 30 ndi 31.