Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Tsamba 32

Tsamba 32

Tsamba 32

▪ Kodi dzina la Mulungu ndi ndani? Onani tsamba 6.

▪ Kodi ndani kwenikweni akulamulira dzikoli? Onani tsamba 8.

▪ Ngati muli ndi ana, kodi n’chifukwa chiyani ndi bwino kukhala ndi nthawi yocheza ndi mwamuna kapena mkazi wanu? Onani tsamba 11.

▪ Kodi mayi amene ankazembetsa miyala ya diamondi komanso kuwabera abwana ake anasintha bwanji kukhala woona mtima? Onani masamba 26 ndi 27.

▪ Kodi n’chifukwa chiyani Mboni za Yehova sizigwiritsa ntchito mafano polambira? Onani masamba 30 ndi 31.